Email a copy of 'Malawi leader appoints new boards:  Full list including CSOs leaders' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

68 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Bob
Bob
9 years ago

Ma appointees enawa ndima hule akawononga ku ma parastatals. I wish akanamapanga background check before appointing them. I know Frank Mbeta who has been appointed pa board ya ku MACRA. He is married but right now he has gone to South Africa for a holiday with a girlfriend, Keiko Msusa. Yemweyo amanyengana ndi Pachalo mpaka the two girls fought for him at TJ’s bar.

lucio mulipa
lucio mulipa
9 years ago

ifenso maudindowo tikuwafunatu

Polofesa
9 years ago

Congrats amnzanga amene tasankhidwa. Tigwire ntchito basi.

Amang'anja
Amang'anja
9 years ago

am just surprised kuti mmene maina achulukiramu dzina lathu ife amang’anja palibepo.
Ife ndi amene tagenda ku boma eti?

Amajta
Amajta
9 years ago

Dean Josaya akufuna abwenzeretse zomwe ayiwonongera Epac FC, awone kusintha amwene.

Kapolo wa Mulungu
Kapolo wa Mulungu
9 years ago

Putting party organising secretary at the hem of ESCOM is a recipe for financial mismanagement of the already struggling parastatal. We don’t want to see ESCOM vehicles taking people for party functions please! I hope your long stay in US was not in vain.

nyamazawo
nyamazawo
9 years ago

Mpaka Abigail !!!!!! Boma ili nde ndilamasanje ndithu

Khadeja Mwima
Khadeja Mwima
9 years ago

FR Andrew Kaufawo muwawuze asiye kuchitila nkhanza ogwira ntchito awo ku TV Luntha ndi Montfort Media komwe atolankhani amagwila ntchito mwamatha chifukwa cha nkhanza za mkulu ameneyu. Ndipo samayenera kukhala mu board ya MACOHA

Patriotic Citizen
Patriotic Citizen
9 years ago

Congratulations guys. I can only wish you well

Kalanga
Kalanga
9 years ago

Kaya zanuzo but congra Namba!

Read previous post:
Robbers attack Muluzi residence, two watchmen arrested 

As insecurity problem rages on in Malawi, a group of armed robbers in the capital Lilongwe beat the security detail...

Close