Email a copy of 'Malawi man arrested for indecent assualt on boy, 13' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi man arrested for indecent assualt on boy, 13' to a friend
Standard Bank Group has revealed in its most recent release that higher interest rates and tough economic conditions in Malawi are...
Utsogoleri wamathanyula
Koma ameneyu bwanji?ma D 7 onsewa sakuwaona , osangopita kwa kachere bwanji ?akathandizidwe, ku wishes, Hip Hop,Town house, kumphasa, kapena ku full dose..ngakhale kwa masapula alipo akazi ongoyenda yakali yakali, umenewo ndi Mwikho mamwene, akaseve basi ku ZOMBA MAXIMUM PRISON.
alomwe alomwe noooooooooophiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiyaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaa!!!!!!!!!!!!
BOKO HARAM yonseyi,ena kumachita kudikilirana kuli kufuna kunyowetsedwa mpaka ena pamzele,ndithu zokuonera galu wachisika iwe.paja kwanu mkuti?
Utiyankhulitsa pakhundu,koma dziko lilidi m’manja mwa agalu eti!!!!!!!!
muduleni zinthu mbuzi adamupatsa ambuyakezo kuti nkhanza zimenezi asadzachitirenso wina kapolo wa chilomweyu
Awone kiama ameneyo abwere LL tidzangomuchotsa katundu wakeyo. Just to curb his libido
Zonsezi ndi APM,there is more to come
Ufiti Eti,,,,,ameneyo Amusekele Ku Ndende De Whole Of His Lyf
Nyere zanji zoukira pa mwamuna mnzako?
Rubish and not fit for human consuption. This devil must go to hell
Koma ndichani a Malawi ufiti eti akazi osewa sakukanaso ameneyo alangidwe basi