Email a copy of 'Malawi MPs receive death threats over illegal wood as police brutalises Jooma’s home' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi MPs receive death threats over illegal wood as police brutalises Jooma’s home' to a friend
Malawi prosecutors have applied to court for seizure warrants for property connected to Cashgate belonging a former junior civil servant...
Salule is also mugulu lomwelo la zigawenga. A Police mufufuzeni uyu. whyy do u fear him!
Owe mbale wake WA masangwi,or fellow family member whatsoever usatinyase kapena kitipsetsa mitima pa nkhani ya kuphedwa kwa chasowa,utsi sufuka popanda Moto,masangwi played a part in chasowa’s murder only that there is justice in this planet especially when it comes to ones in leadership,so zip it or else mmxx.# masangwi brother
Apolisi athuwa koma kuwatuma nkhani ngati zimenezi ndiye amathamanga kapena kuwawuza kuti akagwire vakabu. Anthu okuti akumwela zawo sanabe zamunthu apolisa athu amathamangila amenewo koma kuwawuza kuti wakuba kuno uva galimoto tilibe.
Kkkkk Salule waliliratu imfa ya mafia m’bale wake chokweza asadafe nkomwe e.
Chikwanje, chiopsezo, ndi chanichanichani uko! DPP chiongolero.
anthu akuba awa a dpp; anaononga chikangawa ku North imene inali nkhalango yokongola imene kamuzu anakoza tsopano akufuna kumaliza timitengo tonse tachilengedwe tomwe tinatsala
Nyasatimes Editor I would like to express my disappointment with your online paper for deliberately and willfully publishing comments that are not only defamatory and slanderous to my brother but are also clearly putting his life in danger. I hope you know what your are doing. The fact that you are publishing this online paper from overseas should not give you lincence to deliberately destroy people’s lives and believe you will always get away with it. You have deliberately and systematically painted my brother as a monster in the minds of your readership. You were even the first to tell… Read more »
kodi ku Malawi kuli police? ine ndinagula pistol gun, uta plus nkhwangwa ndizimene ndimazitetezela ndipo ndimayenda nazo mu galimoto mwanga ….. useless police
HAA ACHINA MASANGWI AYAMBAPO KUGWILISA DIRTY HANDS AKUFUNA APHESO NGATI MUMENE ANAPHERA CHASOWA ETI!!!!!
ntchito za Dpp ndizimenezo,awa anapha chasowa pa 2 july anatiphera achibale zinthu sizizayenda kwa awa.