Email a copy of 'Malawi music is laughable, everyone wants to sing like Nigerians –Tutor Chechamba' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi music is laughable, everyone wants to sing like Nigerians –Tutor Chechamba' to a friend
Lilongwe based side Epac FC have said they will do everything possible to boost their squad with the services of...
Vuto achinyamatawa akungotsata zili zose at kufuna mbiri….ndie ndizosanveka zomwe at ndi Muzk kkkkkkkkkkk
Oyimba apa Malawi Mbuzi! ndati ndiwagulira mbuzi posadziwa kuyimba
Bloody copycats
A CheChambawo kodi anatulutsapo chimbale?!Ngati sanatulutsepo achite zimenezo kuti tione kusiyana kwawo ndi enawo. Akhoza kumangotokota zambirimbiri apa. Kukhala tutor wa music sikuti ndiwe dolo odziwa kuimba. Mukhalira beni yemweyo!!
dats truth samtymz u cnt even know dat dis muzic z from Malawi coz thy r jst copying
Izi NDIZOWONA….pali Wannabe ambiri ku Hip hop…Afro Beat ndiye ndi ambiri Tay Grin akapangaFUSE manganje kaya ndi mganda anthu ndikumamuDISSA…..What we lack is originality
Ngati zikutivuta kuyendetsa bwino dziko lathu,what more with music?
@Marcus Zimbiri. Paul Banda or Thomas Chibade are in the minority. The copycats belong in the majority!
Amalawi mbuzi za anthu zeni zeni. they cant even construct a road, they will steal the funds. nobody loves their country. u cant even sing your own soul
yes bcos omverafe lovs export songs
limbani bandayo ndiye asatokote. i’ve never hear a single good song by him. umamudziwa picksy iwe? nanga tay grin bwa? nyo!