Email a copy of 'Malawi Muslims’ leader under attack over abuse of funds' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi Muslims’ leader under attack over abuse of funds' to a friend
Former Surestream Technical Director Peter Mponda is confident that his team now named Wizards FC will do well in the...
IWE IBRAHIM MAKWATI !!!
IWENSO USATIBOWE APA , OLO UTAMANGIDWA ANGADANDAULE NDINDANI ? ZAZIII
MUSAIWALETU PAJA NDINAMANGIDWA CHIFUKWA CHA SHEIKH UMALI OCHI PANO NDI MANGIDWA CHIFUKWA CHAINU
I have no problem seeing Muslim stealing. It is part of their legacy Profet Muhamad left. Mtendere ukhale kwa iye
Mijomba yaliranso ndi cashgate yawo.Kaya situmizilanapo boko haram pamenepa?He he see koma ziliko pamalawi.
KODI SHEHE SALMIN NDI CHAIR WA MAM MAGALIMOTO AMENE AKUYENDERA ANAGULA NDI NDALAMA ZOCHOKERA KUTI CHIFUKWA ANALI MPAWINSO NGATI INE? THESE ARE THE QUESTIONS WHICH NEEDS ANSWERS
BUT EVEN IT WAS DECIDED THAT SALMIN OR KAWINGA CONTEST FOR CHAIR OF MAM SANGAWINE CHIFUKWA THEY ARE SPENT FORCE. NKANI IMENEYI WAYITULUSA NDI SHEHE JAFALI KAWINGA CHIFUKWA ALIBE CHOCHITA NDIPONSO SAKUGAYILIDWA MA ALLOWANCE KUCHOKERA KU MAM. WINANSO NDI MUSSA CHIMBENDE NTOLA NKHANI WAMKULU KWASILAMU AMENE ALIBE NCHITO KOMA KUMADYERA PACHIKAMWA PAKE AKATIGULISA NKHANI NDI ANA AKE ASIKANA AKAPANGA SELL MATUPI AW
IFE ZIKUTINYASA MUKAMALEMBESA NKHANI ZACHISILAMU PA INTENET CHIFUKWA MULIBE UMBONI WOKWANILA
National chair ndi MR pomwe SG ndi Dr. koma yaaaaaa
Musiye kusokosera pa Radio Islam chifukwa ndinu nomwe amene mukutiphunzitsa khalidwe lonyasali.
I only know one clean Sheikh Ali Kennedy and he don’t accept nonses. Pray zat Allah intervens and bring peace among fellow Moslem.
Paja asilamu mumakonda mapokoso komanso ngondo,tamenyanani tionele nawo kkkkkk
SH Idriss MHD mwaiwala zomwe munalonjeza ndimanga Universty Chipatala cha Aslam you evin promised kuti ndibwino kuti muzizakwera mamin bus koma muzasamala chuma cha Asilam today you are driving porsh cars ndinu odala ndyerani Chisilamu mmene mungathere but 1day you wil Answer pa maso Allah sinu nokha ai koma aliyense yemwe chuma chake chikukhudzana ndi ndalama Zachisilam ndiotembeleledwa Masheikh akumalawi chonde chitani manyazi chisilamu mwachidyera kokwanira plz plz tapanganiko zoti mawa ana athuwa azaone kusinthako taonani mipingo ya anzathu moti inu omwe muli atsogoleri a MAM simupanga manyazi ?