Email a copy of 'Malawi opposition maintains ultimatum on food, economy' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

9 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Mkulinga utamva
8 years ago

Game on! Ulibe zeru. Akumwera ngati akulima ndikonko kumwera osati Ku central. Ifetu Ku Central ndiye ntchito yathu kulima inu koma tea chimanga mukuphunzira pino kulima. Enanu njala mudaizolowera koma ife ndimdani. 2019 onse akufunira dzikolawo zabwino ndi Chakwera! Chakwera! Chakwera. Osalikonda dzikoli ndiye zinazo!

cashgate
8 years ago

uladi mussa ukuyendesa chipani cha masiye cha pipi chomwe ng’ombe yaikaz yako inakuthawilan

Bwanje North
Bwanje North
8 years ago

Chaka cha 2014 chinali chomwe MCP ikanalowa m boma. 2019 musazinamize a Opposition this lomwe akuzawinanso mopanda kukaika.

checky okwey
8 years ago

Kwayemwe ali m’Malawi muno waziona chaka chino chizadziwe ndi chipande poomora 2019 ndepoti mumsdziwa kubera zabeleniso

Game on!
Game on!
8 years ago

Number 1 ukunama amenetu tikulima kuno ku Central ndi ife a ku Mwera. Kodi Uladiyu mmene make namaloko amagulitsa chimanga ndi ndege ndikuba za oil ndikunena kuti akumudziwa amene adamuombera mphwiyo iye adali kuti? Koma camapign 2018 ife a DPP tidzayenda moyera chifukwa akapilikoni ofuna kulowera pawindo dziko lonse ngakhale mafumu a kwawo kwa Chakwera yemweyo akuwadziwa. mukucheperatu inu tikafika potopa ndi ulemu tikupatsani ultimatum kuti iyambike ya game zikwanje tione amene angabalalike kuMwera mukunyozako.

chimstamusani
8 years ago

a Uladi mumatha kulankhula koma vuto ndilakuti mabodza anu tidawatulukira kale.

chimstamusani
8 years ago

a Uladi zanu zinada kale.Akakamizeni aboma pofuna kuthandiza a malawi,osati kuti a malawi akopeke ndiinu.Ife ndi nganganga ndi APM.

BOKHO
BOKHO
8 years ago

How can someone say will defeat opposition thoroughly yet day by we see insecurity in the country, hunger, shortage of drugs in the hospital, high inflation, rising of prices of commodities recently petrol, dwindling of education, high corruption in DPP government please go and rest in peace come 2019.

pido
8 years ago

Njalayitu ikadakhala njala akdakhala kuti chimanga sichikupita ku Mwela ku Thyolo, Chiradzulu and mulanje. Popeza akumipandowo akutenga chimanga through ADMARC kukagulitsa kwaoko they say kulibe njala. Someone realyy from BT said anthu nonse mukunama. Kunja kuno kulibe njala. If kummwera tikudya bwino. Central, North and East musagulitse chimanga chaka chino kwa mavenda and ADMARC tione komwe anyani amenewa atakadye. Anthu osagwira ntchito koma kuba basi

Read previous post:
Louisa Kabwila’s paternal family is DPP: Ministry says sacking not politically inspired

It has been established that daughter of Malawi Congress Party (MCP) spokesperson Jessie Kabwila who has been sacked barely a...

Close