Email a copy of 'Malawi opposition maintains ultimatum on food, economy' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi opposition maintains ultimatum on food, economy' to a friend
It has been established that daughter of Malawi Congress Party (MCP) spokesperson Jessie Kabwila who has been sacked barely a...
Game on! Ulibe zeru. Akumwera ngati akulima ndikonko kumwera osati Ku central. Ifetu Ku Central ndiye ntchito yathu kulima inu koma tea chimanga mukuphunzira pino kulima. Enanu njala mudaizolowera koma ife ndimdani. 2019 onse akufunira dzikolawo zabwino ndi Chakwera! Chakwera! Chakwera. Osalikonda dzikoli ndiye zinazo!
uladi mussa ukuyendesa chipani cha masiye cha pipi chomwe ng’ombe yaikaz yako inakuthawilan
Chaka cha 2014 chinali chomwe MCP ikanalowa m boma. 2019 musazinamize a Opposition this lomwe akuzawinanso mopanda kukaika.
Kwayemwe ali m’Malawi muno waziona chaka chino chizadziwe ndi chipande poomora 2019 ndepoti mumsdziwa kubera zabeleniso
Number 1 ukunama amenetu tikulima kuno ku Central ndi ife a ku Mwera. Kodi Uladiyu mmene make namaloko amagulitsa chimanga ndi ndege ndikuba za oil ndikunena kuti akumudziwa amene adamuombera mphwiyo iye adali kuti? Koma camapign 2018 ife a DPP tidzayenda moyera chifukwa akapilikoni ofuna kulowera pawindo dziko lonse ngakhale mafumu a kwawo kwa Chakwera yemweyo akuwadziwa. mukucheperatu inu tikafika potopa ndi ulemu tikupatsani ultimatum kuti iyambike ya game zikwanje tione amene angabalalike kuMwera mukunyozako.
a Uladi mumatha kulankhula koma vuto ndilakuti mabodza anu tidawatulukira kale.
a Uladi zanu zinada kale.Akakamizeni aboma pofuna kuthandiza a malawi,osati kuti a malawi akopeke ndiinu.Ife ndi nganganga ndi APM.
How can someone say will defeat opposition thoroughly yet day by we see insecurity in the country, hunger, shortage of drugs in the hospital, high inflation, rising of prices of commodities recently petrol, dwindling of education, high corruption in DPP government please go and rest in peace come 2019.
Njalayitu ikadakhala njala akdakhala kuti chimanga sichikupita ku Mwela ku Thyolo, Chiradzulu and mulanje. Popeza akumipandowo akutenga chimanga through ADMARC kukagulitsa kwaoko they say kulibe njala. Someone realyy from BT said anthu nonse mukunama. Kunja kuno kulibe njala. If kummwera tikudya bwino. Central, North and East musagulitse chimanga chaka chino kwa mavenda and ADMARC tione komwe anyani amenewa atakadye. Anthu osagwira ntchito koma kuba basi