Email a copy of 'Malawi opposition raises concerns over death threats: ‘Stop being critical to President or you will die’' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

19 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
zebron henry banda
zebron henry banda
8 years ago

Trying to intimidate people in opposition is not a solutIon malawians want to hear.malawians want tangible solutions from the multiple problems they face by their government.assassinations of those officials is plain stupid and dangerous.the backlash from that could see you,the perpetrators,a mass-hunt by the populace to kill you too.Solve the damn problems,no threats!

Cash Gate
8 years ago

Ngati Boma Likudana Ndi Kudzudzulidwa Ndiye Kuti Anthu Amene Akuyendetsa Boma Sakudziwa Kuti Democrancey Ndi Chani, Mmenemu Ndi Mmene Dziko La Democrace Limayendera, Or Muphe Anthuwa Dziwani Ndithu Kuti One Day Mudzakhala Kunja Kwa Boma, Sindinu Amuyaya Ayi, Yendetsani Dziko Ndi Chikondi, A Opposition Mutawamvera Zomwe Amanena, Mutha Kuchita Bwino Ngati Momwe Anachitira Bwino Malemu Bingu Mu Zaka Five Zoyambirira Zija, Anayigwiritsa Ntchito Opposition,

fred
fred
8 years ago

come what may, forces will force matters

lets shame the devil.say no to demo

say no to suffering

say no to madeya, love nsima

say no to treason

say no to groaning

pray to God for help

He become concerned when the children are suffering. exodus 2 :23

he become attentive to the cry of the isralites.

is Malawi genuinely crying?

lets turn to God
God will fight your battles
God Bless Malawi and its leaders, be it in power or in opposition

PAYERE PAYERE
PAYERE PAYERE
8 years ago

Peter akupha wa opposition lizamuweluza ndi dziko lonse la pansi chifwa alindiasilikili ndiponso police , chiweluzo chake ndi kunja kwa Malawi ndiye achenjere ndiponso awone kusiyana kwache , zimene akupangazi ndimasewera. Wachepa Peter opposition itha kumugonjetsa ndi kachipani kache ka 34% .

mkaidi waswagga
8 years ago

mbuzi iwe osangozisiya bwnj….. zimafuna olimba mtima izi osat kukamwa ngat wapana mwanaliye choncho

Chilungamo Chimawawa
Chilungamo Chimawawa
8 years ago

dpp is a party of thugs, they are still thugs and will remain thugs!!!!!!

bristol
8 years ago

DPP is a helpless and clueless party. No wonder they are threating lives of opposition leaders because they are new to Malawi – they never fought for freedom during early 90s. they are there to enrich themselves and not serving the interest of Malawians. They did not win 2014 but rose to power through head of electoral commission and not by votes. 2014 was a rigged election even children know this – why did a big person weep during announcement of the winner, he knew he had betrayed innocent Malawians.

mzungumbuli
mzungumbuli
8 years ago

“Mwamuna mzako m’pachulu n’kulinga utakwelapo” Agalu inu a DPP muyerekeze kuchita zamanyi zanuzo, chimunthu chanu chopanda mano nkamwacho chidzagwa ngati nkulu wake uja, fotsekiiiiiiii !!!!!!!

levelheaded
8 years ago

How many have so far died out of these so called death threats?

Every office has its own challenges, don’t you know?
You are calling the president to step down. Do you think that those who voted for him can just leave you like that?
Zimatiwawatu kwambiri, kapena simunamveko kuwawa kwake eti?
Yesetsani campaign, mukadzawina zisankho a PP kapena MCP mudzamveko kuwawa kwake anthu amene sanavotere Chakwera akumuwuza kuti atule pansi udindo.
Inuyo amene mwavutikira kumuvotera tiwone ngati mudzangokhala duu.

mjomba welewo
mjomba welewo
8 years ago

Enanu tidzaka titatu tapitatu munasauka nkumavala timajinzi tothina mtaunimu anthu kumati kodi ndi auje awo mukuyenda khwekhwelekhwekhwele zitakusokonekelani…pompano musaukanso muwona…munasakha game yachabe…mukulimbana ndi Kabwila munthu wophunzila bwino osati kuphunzila kongogulanazo mapepala…kumangolankhula english yoloweza basi…tima vocabulary toloweza basi…zaziii…ine mjomba ndisazakuoneni muli deludelu kulowela kunyumba ya Kabwila kuti akupelekezeni kwa Bigman Chakwela kuti akakupepetseleni mutavalanso kajinzi kothina…

Read previous post:
Blue Eagles Sisters at top of  Central Health league

Blue Eagles Sisters send a warning signal in the Central Health Lilongwe and District Netball League on Saturday as they...

Close