Email a copy of 'Malawi Pentecostal pastor jailed 7 years for sexual assualt tean girl' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi Pentecostal pastor jailed 7 years for sexual assualt tean girl' to a friend
Many times people have prayed to God to intervene in situations but have at the same time put full dependence...
anyapala apatapo m’busa apa kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk
Malawian women, lets learn to behave. zinazi timaziputa dala
Sad
ku mpoto ndi choncho.mixxxxxx
Wrong decision from a FOOLISH Mother.How DARE SHE GIVE HER DAUGHTER LIKE THAT? IS THAT WOMAN HAVING A HUSBAND? HE WUD HAVE CRASHED THAT STUPID IDEA. SHE MUST B A LONE.APATU ANAPEREKA MWANAYO.KUNGOTI ADAPITA KU POLICE KUOPA KUTI ANGAWONEKERE NG’AMBA KWA ANZAWO NDIYE MANYAZI AWAGWIRA.
Tikuferanji timverayi hatiphunzitsa’ë? Chonsecho mayii ankadziwa kuti munthu wabambo atokhala yekha. nkupititsa dala mwana wakazi kumeneko ankatofunachani?
Asadadaule komanso a koti mutomutchaja zaka zonsezo amene atalele mimbayo ndani? nangamwana akabadwa atasamale ndani?
Che Patricia, munepo chani? chifukwa pamenepa ayenera kuphunzitsidwa ndi mayii chifukwa ankapanga zadala.
M’busa sanalakwitse anampasa dala mwanayo nde iye anakatani pamenepa ndi sex basi panalibeso kuchitila mwina. Atuluke ameneyo ndende!
Zadala izi mayi akewo amamupeleka okha mbusa naye nkuzango gwira tchito yotamandika.
mai wopusa ameneyu,m busa ndi munthu alinso ndi zilakolako za thupi.Nawo akulu a mpingo anali kuti osampasa mnyamata kuti azikamuthandiza m busa? Za dala izi.
We dont if this was really a man of God. Thiis was nt a pastor trust me. Psalms 1 v 1. If he were a pastor could have made judgement. He deserves stifer punishment ft disgracing pastors , believers. Azibusa tengeraniponi phunziro. Wachamba akuposani chifukwa sakhala ndi nyere ngati iyo iwe mubusa wa damager