Email a copy of 'Malawi Police arbitrarily shot and kill two in Lilongwe' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

62 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
ngwazi ya ufa
ngwazi ya ufa
8 years ago

In countries like South Africa a shoot to kill is implemented when criminals have fire arm pointed at police officer, but in countries like Malawi, shoot to kill is for what?

myamiko matapa
8 years ago

Koma akapha wapolice ndiye mumakondwa

A Micky
8 years ago

We are living in fear because of thieves and armed robbers. If what people are saying is true, then we should not politicise issues here.l Policemen are at work

Elisha
Elisha
8 years ago

chonde asiyeni apolisi agwire ntchito yothana ndi mbava, luka ndi kawongayo zinali mbavazoospya musanyoze apolisi musalowese ndale pa nkhani zambava, tafusani pa vinthukutu zambava zimenezi kuchilumba

First offender
First offender
8 years ago

Ngati uli mbava sulimba ngongole yokatenga usiku yamtundu wanji and moreover mukudusanso kumandanso mbava ndi zomwezo it’s not a mistaken identify.

First offender
First offender
8 years ago

Ken msonda ngati nawenso uli mbava tasala pang’ono kukushuta wamva?

kamfana
8 years ago

MHRC,also document the killings of Police Officers & Innocent Civilians by these SAME CRUEL ROBERS.

Rejoice Kachana
Rejoice Kachana
8 years ago

Iwe Ken Msonda shut up

Peterson
8 years ago

Ndikuyamika ntchito yabwino yomwe a Police mukugwira yokupha anthu osakonedza dziko. Komanso musamanyang musamayang’ane nkhope ayi chifukwa enawo ndi abale anunso.A cash gatenso aphedwe mosayang’anira nkhope

Rejoice Kachana
Rejoice Kachana
8 years ago

Inu anthu musavutike an amenewa ndi mbava zoopsa ask anybody wa ku chilumba akuuzani za ana amenewa achi Kawonga mbava wina amwabera uncle ake a mwenelupembe Kawonga mbava yoopsa.tapitani ku Chilumba pafupi ndi galison mukafunse za ana amenewa.Peolpe are rejoicing …kaya winayo watsitsimukiranji ….ma nurse ndi ma doctors tachitani naye ameneyo

Read previous post:
MCP boost! Chakwera welcomes back Gwengwe, Kayembe, Zulu, Kalazi Mbewe

Malawi Congress Party (MCP) president Dr Lazarus Chakwera on Sunday welcomed political prodigal members back in MCP fold at a rally which...

Close