Email a copy of 'Malawi police arrest man for scorching step son for wrongs of mum' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

29 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
fanizo mbwana
fanizo mbwana
9 years ago

Minyama ikafuna kukutsata you never know

chambo
9 years ago

Alcohol is not adefence he had an intention already and is deserving stiff punishment for others yo take a lesson.

King shafick
9 years ago

ONCE balaka alwayz balaka kumudzi kwathu ndimakunyadira tiyeni tonse anthu akubalaka tizunguze 2015 kuposa apa

STABLE
9 years ago

Tatopa ndikumva nyasi za kubalaka.

LUCIOUS MANDA
9 years ago

Inu kodi kumeneku si kwawo kwa soldier woimba uja? Nanga bwanji osapanga za u soldierwo kumeneko ndi anthu akuvuta ndi za usaveji zo.

Achisale Kumangoni
Achisale Kumangoni
9 years ago

Kodi Asilamu mwayamba kumwa nao mowa wathu uja eti?? Mwaona vuto lomwa mobisika?

KHWITCHAVIZO
9 years ago

kachasuyo anali wongolengela Zomba basi ,mission inali ya mfana yemweyo,asaname.

the Northern speech
the Northern speech
9 years ago

Ndiye balaka imeneyo

christopher guma
9 years ago

Zilibwino kuti wamangidwa. Ngati ndi mowa achimina.These kind of pple tarnish the image of our nation. Zaka 32 kumaganiza mopepera ngati khanda?

yamikani
yamikani
9 years ago

Balaka!!!! Kwao kwa Getrude uyeni.

Read previous post:
Malawi Police says bank robbery suspect still married to cop

Police in Malawi have revealed that Pelekani Malunga one of the arrested suspects in the K100 million bank robbery is...

Close