Email a copy of 'Malawi Police arrest two for robbing a boss' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi Police arrest two for robbing a boss' to a friend
In a bid to support increased access to education by girls, premier mobile network service provider TNM is offering free...
apolice nanu
Bravo! Well done the cops that’s why it was decided that police must mount roadblocks cos of thieves like these two foolish young men who thought that they could steal from somebody who gave them a job. Foolishness!
Mbava kubera mbava, mbava ndikuzagwira mbava shaaa mbava zosakondana kkkkk
should they be promoted for what ndi Mulungu wawayalutsa akubawo. mwina zinthu zina abisa a polisiwo. m’mayesa a polisi nde mbavazo. kutereku kugwira akubawo ndi jealousy akufuna akanaba iwowo. praises should go to God for unveiling the plan
Apa zikukhudzanso mtundu? Umafuna akwate chemwali ako kapena amako ndiye uyamikire?
Mbava zaberana mbava zokhazokha.Poti Mra nayonso yazadza ndi mbava zokhazokha.
ndamenewo akuvutitsanso kuno ku Lilogwe amen ,ewo tafusani bwino tawafusani bwin ,o lomwe
Okuba alibe malemba, olo bwana wawoyo ndiyenso mbava n¤#1 olo kumufunsa kuti awonese makata apezeka kuti alibe a police gwilani ntchito
Kuba katundu wanyumba mpaka kukakwela naye minibus. Oh osango nyamulila mu wilibala bwanja madolo awaso nawo
WA zaka 23 ndiye kuti wamaliza sukulu kukayamba ya m’gwanya Malawi Yasautsadi nanunso a boma muyamba liti ma community college aja taonani zomwe akuchita achinyamatazi tsopano any way police well done