Email a copy of 'Malawi Police officer did not leave suicide note before fatally shooting himself' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

15 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Chosambava
Chosambava
9 years ago

Constable keeping fire arm at his house..rubbish

wakuba
wakuba
9 years ago

DEY ARE ALL FOOLS,PSYCHOLOGICAL SKILLS IN THEM

nkhoswe
9 years ago

no smock without fire. need deeply investigated and will find the cause.

Young B
9 years ago

A very week we r hearing of crime issues done by police officers,lol wats happening to our mobile forces?hav they lost their morals??

Young B
9 years ago

A very week we r hearing these issues of crimes done by the police officers,lol where r their morals

Kwame
Kwame
9 years ago

Bambo Chisi nkutheka anaphapo mkayidi pomuombela nanga si amakhala ndi mfuti ndiye mzimu wa munthuyo wakhala ukuwalonda bambowa. Anthu ena amakhala okhwima mu zisamba paja nthawi zina mumbuyomo zimamveka kuti akayidi aphedwa koma sizimaululika kuti amawawombelayo ndi ndani. Amalawi iyi nkhani ya a chisi yazunguza anthu ubongo. Munthu kuwombela ana ake okula kula mumaso muli gwa siyogwila chilipo chilipo. Bola kukanakhala usiku zikanamveka kuti mwina amayesa akuba nanga si anawo anali anyamata. Koma likuswa mtengo basi kulowa kuchipinda kukayitenga mfuti basi pho again pho ali ayi ndikapheso winayo pho ayi tonse tadabwa. Bola kukanakhala kwa azunguko kapena ku joni komwe… Read more »

Charles Elias
9 years ago

mbava ndizomwe amakonda kuzilemba ntchito ku police, ukawafunsa ati send a thief to catch a thief.

iPhone Kaunda
9 years ago

Police yidapita ndi Kamuzu ndi IG Kamwana

MELINDA
MELINDA
9 years ago

Machimo akachuluka ,zotsatila zake zimakhala zimenezi.nde kuti munthuyu amafunika counselling komanso deriverance, koma analibe omuuza.

Tiyeni abale tikamadzudzulidwa ndi anthu ena,tizidziwa kuti Mulungu akutiyankhula,ndi bwino kusintha zisanafike poyipa.

Imfa ya munthu ochimwa,Mulungu samasangalala nayo.

Manyi Sabedwa
9 years ago

Aliyense amakolola zomwe wafesa this country is full of satanism izi ndizomwe tidafesa sitinati ntchito ndiyosayamba

Read previous post:
Malawi Police Service needs more than prayers

 A flurry of incidences that have punctuated the Malawi Police Service (MPS) lately are as disturbing as they are depressing....

Close