Email a copy of 'Malawi Police quiz MP over Admarc maize smuggling' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

10 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
true kaweri
true kaweri
8 years ago

Bvuto ndiloti kumalawi anthu andale amangofuni kupenza chuma cha banja lao kwatha.chimanga chaku admarc si cha dpp,or zipani zosusa,koma ndi cha boma.Zipani zikafuna kupereka kwa anthu awo wo wasatira akaode chao osati ichi.zinthu zimene mkuchitira anthu amalawi muzakolora mbeu yanu.Anthu azibvutika inuyo mtapasana chimanga cha boma,kenanka osamangidwa ndikulimbana ndi cashgate ya kale,pamene imeneyo ndi cashgate yoopya kubera anthu chimanga munthawi ngati imeneyi yobvuta njara mpaka ku likoma thini lafika pa k5,800,pafui k6,000.Chimanga cho si cha Dpp,koma cha amalawi ndrama za boma,boma ili ndi la kubanso kwa mbiri cashgate,koma ndilochenjera kaamba ka president.

Wakwathu Mwana
Wakwathu Mwana
8 years ago

So bad and unfortunate for beloved brothers and sisters in ntcheu. 100 bags for only one constituency instead of reaching the many hunger stricken citizens of ntcheu boma area. Now all those who are sleeping at the depot shall go home without any single grain. Thats being insensitive and irresponsible for the MP.

Chekacheka
Chekacheka
8 years ago

What is Felix Jumbe trying to say? The last time he stood on the hill and aploud gvt that it has enough maize on stock, people should not panic, today people are spending 4 days just to buy 10kg of maize, is that not paniciking? For Mwayi Kamuyambeni, my former paster, DPP is where you belong, its where your fellow killers belong

Kamdelero
Kamdelero
8 years ago

Mwati District Governor’yo ndan? Nanga MP’yo ndani? My foot!!!!! Zofuna a Malawi.

daudi mj
daudi mj
8 years ago

Love of money is the root cause. Our politicians make me laugh if they are really there to serve people kkkkk. Now we are able to judge on our own. That is why there is voter apathy. People have lost trust

Apostle Kennedy Maluwa
Apostle Kennedy Maluwa
8 years ago

Its too bad for the Malawians, this is January what about February? Lets pray to God for good readership.

Man of God
Man of God
8 years ago

A Jumbe mwatani kodi? Inu nomwe munaima pagulu ndi kumayamikira boma, kumati lagula chimanga chokwanira kotero kuti amalawi tisadere nkhawa. Tsopano lero mukutinso chiani? Msuzi watha?

Thochi
Thochi
8 years ago

THE Government should declare no sale of maize by anyone but Admarc. This will solve all problems. Malawi does that chimanga anthu akayamba kudya chikakhwima mmunda. Amati no chimanga chowotcha kungulitsa pa nsika.

2016 welcome
2016 welcome
8 years ago

A sick society but always claiming to be God fearing.

Ibu wa Mutharika
Ibu wa Mutharika
8 years ago

The MP is DPP no wonder they have treated him with kid gloves. This buttresses the argument that those in the high echelons of power are spared. Cry beloved Malawi.

Read previous post:
Silver Strikers sign two players from Wizard: Bright Munthali and Levison Maganizo

Silver Strikers have become the second team to invade Fisd Wizards camp following their completion in signing midfielder Levison Maganizo...

Close