Email a copy of 'Malawi prison boss shoots dead two sons, arrested: 5 nabbed for cop’s murder' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi prison boss shoots dead two sons, arrested: 5 nabbed for cop’s murder' to a friend
Mobile telecommunications operator Airtel Malawi gave testimony in the shooting of former budget director in the Ministry of Finance Paul...
Eeeeeeeish awatu ndiye achachanda, ndipo ndiye alindi chandamale, samaphonya, take cover,komaso mumufufuze ameneyu ngati wachitira izi mikozo yake yomwe , kulibwanji akaidi waphatu phwiiii .
I Support The Father.Ana Anamutopesa AWa
Could Nat Be The First Time
Achita bwino kuwapha apuludzu amenewa, ana amwano, makani, nkhwidzi,osamva,uhule
Zamwano mnyumba mwa makolo basi! Iyaa! Ndiponso akanamupha ndi Lusungu wamkazi
Yemweyo,aaa! Ana ochita kutopetsa chonchi? Ndiye ana mpaka kumera dzindevu koma kumakhala ndi makolo awo, bwanji osakwatira? Usilu basi! Makolo enanso muchenjere zilombo mukusunga mnyumba mwanuzo! Koma 2015 kuli zinthu!
It aint an easy thing to stay with parents when your a grown and doing nothing so the best thing is to use your charnces while still young…so that atleast you should have something to do in future.
Azibambo aulesi osagwira ntchito koma kulawirila kukangana basi,ana opusa akuyenera kufa ndithu 29-23 alibe m’manjamwamakolo ana opusa ause muntendere.wokuphayo alagidwe molingana ndimalamulo wokhudza kupha.
Poor Chisi, why? However Pliz understand this old man. Makosanawa anakula ndipo amasowetsa mtendere.
This aint fair
Akuluakula amenewo mukafufuza mutsyre madalawo, anatopa nawo anawo.
Lesson to unruly children,at twenty something kumakhalabe ndi makolo,wina yonso akuti anangosiya ntchito ku prison why?madalawo ofunika bail,my opinion
Akuyenera kulandira chilango basi,vutoli analilekerera poyamba