Malawi Revenue Authority impounds 42 kilos of Indian hemp in Mzimba
The Malawi Revenue Authority (MRA) intercepted a truck and seized Indian hemp weighing 42 kilogrammes (kgs) at Lojwa, just after Jenda Trading Centre in Mzimba District.
The incident occurred on Thursday, February 5, 2015 following a tip to MRA from members of the public about suspicious items in the truck.
The Indian hemp was in a carton and divided in 6 packages, each weighing 7kgs. The carton was concealed between sun-dried small fish locally known as Matemba.
The owner of the consignment was identified as Christopher Mkuwu from Mangochi District. Mkuwu was immediately arrested and taken to Champhira Police Post.
MRA is further appealing to members of the general public to always report issues of any malpractices such as smuggling, tax evasion and corruption through the toll free number 847 for Airtel and TNM subscribers or 80000847 for MTL subscribers.
Informants can also send their tips to the Centre through email address: [email protected] or fax to 0182 229.
Follow and Subscribe Nyasa TV :
Mbuzi za custom zikungolephera target ntchito kuba basi mukulimbana ndi zimenezo.
Back pulling,ogolitsa ziwaro ndiye sport free,che mtira mmmxxx where is nacipanti?
Va ziii! Kumupatcha galu wakhoza kulavula.
In fact the poilce know dealers in chilobwe,ndirande and kameza and they just collect tithe
mukatero mukagulitse ndinu ngati mwaoda. …mzanuyo ndiye wachita kugula ….wina ndizamuombera ndimfuti yake yomwe ine
Mra pamozi ndi apolice amene ali ku mra akugwila ntchito yotamandika kwambili koma vuto lilipo ndilokuti pakakhala mapulomoshoni amene amapasidwa ndi anthu okuti ndi ana. amabwana ntchito salimbikila ,komanso amapezeka mwina angochokela kumene ku school kungofikila ku pulomotedwa .pomwe olimbikila ntchito osaganilizilidwa.Bwana IG,Bwana mwapasa aganizileni ana anu makamaka ku MRA timakunyadilani ndipo ntchito tigwila nanu.
Tawasiyani anthu akagulitse inu! Akakudyereni kuti anzanu mmene pavutira pamalawi?
MRA? Not Police? Paja Njoka timapha kumutu osati ku mchila, mumupane anakaoda kuti mukapezako chamba chambili mwanva? Uyuyu ndiosalakwa ayi he is doing what he knows Best, ndiye mwina amatha yachambayo ndiye mumudyetsela banja lake amene akulima alipo? Brute MW Police and MRA, katundu angodutsa wa amwenye osalipila mukulimbana ndi mmalawi mzanu uyu, Stupid.
Why waste your meagre resources on this man when you could have impounded lots of tons at the Matafale Memorial Show in Chileka Blantyre. And this was in full view of the Police. Za double standards basi!!!!!!!!!!!!
aaah akupangiranji zimene a MRA, they should have waited for the product to fetch market and in return they should get their tax………..simple