Email a copy of 'Malawi Revenue Authority  impounds 42 kilos of Indian hemp in Mzimba' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

22 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Gwaladi
Gwaladi
9 years ago

Mbuzi za custom zikungolephera target ntchito kuba basi mukulimbana ndi zimenezo.

BOX 13 BILILA, N U
9 years ago

Back pulling,ogolitsa ziwaro ndiye sport free,che mtira mmmxxx where is nacipanti?

Likoma Economist
Likoma Economist
9 years ago

Va ziii! Kumupatcha galu wakhoza kulavula.

Weakliks
Weakliks
9 years ago

In fact the poilce know dealers in chilobwe,ndirande and kameza and they just collect tithe

fire man
9 years ago

mukatero mukagulitse ndinu ngati mwaoda. …mzanuyo ndiye wachita kugula ….wina ndizamuombera ndimfuti yake yomwe ine

nyapapi
nyapapi
9 years ago

Mra pamozi ndi apolice amene ali ku mra akugwila ntchito yotamandika kwambili koma vuto lilipo ndilokuti pakakhala mapulomoshoni amene amapasidwa ndi anthu okuti ndi ana. amabwana ntchito salimbikila ,komanso amapezeka mwina angochokela kumene ku school kungofikila ku pulomotedwa .pomwe olimbikila ntchito osaganilizilidwa.Bwana IG,Bwana mwapasa aganizileni ana anu makamaka ku MRA timakunyadilani ndipo ntchito tigwila nanu.

Dzoneni
Dzoneni
9 years ago

Tawasiyani anthu akagulitse inu! Akakudyereni kuti anzanu mmene pavutira pamalawi?

Yankeez
Yankeez
9 years ago

MRA? Not Police? Paja Njoka timapha kumutu osati ku mchila, mumupane anakaoda kuti mukapezako chamba chambili mwanva? Uyuyu ndiosalakwa ayi he is doing what he knows Best, ndiye mwina amatha yachambayo ndiye mumudyetsela banja lake amene akulima alipo? Brute MW Police and MRA, katundu angodutsa wa amwenye osalipila mukulimbana ndi mmalawi mzanu uyu, Stupid.

General Aididi
General Aididi
9 years ago

Why waste your meagre resources on this man when you could have impounded lots of tons at the Matafale Memorial Show in Chileka Blantyre. And this was in full view of the Police. Za double standards basi!!!!!!!!!!!!

Fleshly
Fleshly
9 years ago

aaah akupangiranji zimene a MRA, they should have waited for the product to fetch market and in return they should get their tax………..simple

Read previous post:
Nsejjere offers K10m for Malawi league: SRFA champs to get K7.5m

Sports outfit Southern Region Football Association’s new sponsors Nsijjere have announced that the league champions would pocket K7.5 million for...

Close