Email a copy of 'Malawi ruling DPP wins by-polls, add two MPs' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi ruling DPP wins by-polls, add two MPs' to a friend
Zodiak Broadcasting Station (ZBS) has unleashed another first in Malawi; Family Brains Showdown, an unprecedented thunderbolt television family edutainment masterpiece...
DPP ndi machine dala!!
Zamkutu basi DPP ndiye boma len ileni mu 2019 Dpp idzatenga ma seat 173 enawo adzagawana otsalawo.ck woyee,chapananga woyee,changoima woooooooooyeeeeeeeeeeee
Kumeneko ndiye kubwera booo! DPP WOYEEEEEEE! Prof APM woyeeeee! – CONGRATS!
Amalawi when shall we stop the tribalist bickering. sizitithandizatu zimenezi. timange Malawi with people who can lead our country with passion and deligence.Remember, there will be none outside our Malawi that will come to rule us. Ine zazigawozi zimandinyasa ndi ndikunditopetsa koopsa. Tikumutaya tokhatu malawi. tikuchedwa nazo zimenezo. lets rise above partisan politics and build our nation.
othere countries akutiwerenga kuit kwathu nkukangana. tiyeni tizilimbana ndi ma investors kuti kodi ndi chiani angapangire Amalwi, nanga mpati tili loose kuti dziko lathu liyende bwino osati ati hee achakwera, a msowoya, peter. nzachabechabe zimenezo abaleinu.
tiyeni tikhuzumuke
ine kimva kukoma basi DPP the party of the people
Ine ndine wa chigawo cha pakati. Ndinavotera MCP. Ndimakonda MCP. Congratulations DPP kuti mwaiwina, apa zasonyeza kuti anthu akukondani apa zobera ndikukhulupilira kuti panalibe. Ndimakonda chilungamo tha is why I am congratulating you the DPP koma ndimakonda MCP. Chenjezo kwa inu anzanga nonse a MCP and especially the Centrals. Chakwera wants to sell us to the mortherners. northerners ndi anthu odzikonda, they just want to use MCP through Chakwera za Fedralism. Mulekeni Chakwera adzathandize the northeners koma ife ayi, Chakwera akulamulilidwa ndi mkazi wake nya Kayira wa ku Rumphi ndichifukwa chake anasankha Msowoya kuleka kutenga a Sidiki Mia kapena a… Read more »
Chakwera is a hopeless hope for MCP ndipo sandzalamulira Malawi koma palibe chifukwa kukwatira mai Nyakaira she is a well mannered lady with natural looks a good example and good model for all the skin bleached crew
I am sure you don’t come from the centre and I can understand the pain you are taking to convince the chewas that they are better off with the lomwes. Unfortunately the chewas are neither comfortable with the Nyika nor the lomwes. You are all useless where developing a country is concerned. The tumbukas are good clerks and lomwes make good manual workers and policemen. Oh ooh and good thieves too. Federation is a waist of time Chewas please come back home. You southerners and northerners go home. You mama is lonely. GO HOME GO HOME GO HOME……..
Mbwenumbwenu, learn to respect your friends. This should not be a platform to insult people.
You mbwenumbwenu kutukwana anzanu? learn to respect your friends
Next tifuna referendum ya Quota System kenako federalism tiwone maganizo a Malawi. Nanga si inayamba ndi quota system before the so called federalism?
D phi phi boma ilo