Email a copy of 'Malawi teachers to strike on Sept 5: ‘No reverse gear’' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi teachers to strike on Sept 5: ‘No reverse gear’' to a friend
Malawi’s leading and multi-award winning online news source, Nyasa Times on Saturday night celebrated its iconic 10 years of existence and service...
BRAVO TEACHERS!!! We Malawians in diaspora strongly and wholeheartedly support you for taking such comprehensible action to demand for your rights.The government cannot standup and say it has no funds while at the same time,it hires private jets worth millions of dollars to transport illiterate tribesmen and women to the USA,hiring good for nothing so-called Presidential advisers,exporting Chikangawa logs to foreign countries without government’s knowledge and the funds channeled to private greedy criminals in league with senior government officials while the North is swimming in the waters of inferno and government Medical Stores are exposed to empty shelves attributing to… Read more »
Aziphunzitsi ndi boma lanu ili ndalama munadya towards 2014 zija akutenga eniake akufunani 2019
Ndalama zolipila aziphunzitsi ndi zija anagwilitsa ntchito pipita uku kumtunda kwa Malawi ko!!!!!! MAYI MALAWI
Talk whatever you want but the issue will solve itself in 2019. Mzanu ali pheee chifukwa mavoti ake wodzadza migolo akungodikira. Aziphunzitsinu ndi womwe mukuzunzaso ana athu m’midzimu kumangoti pang’onong’ono ndalama ya chakuti ,mawa ndalama yachakuti, anthu akuba inu. 2019 ikubwera ndi yomwe idzaseve wosati kumangobwetuka akakutumuna azipani zanuzo. Munayamba kupanga ma strike kalekale kuyambira boma la Muluzi koma palibe chiopsezo chomwe chinagwira ntchito kuti nkugwetsa boma. Ndiye ili lingagwe chifukwa cha inu. Every organization has its affliates torwards different parties, so don’t think because you feel pains then all teachers are against this govt. Everyone likes money that is… Read more »
I thought unena za nzeru kkkkkk zikugwirizana bwanji,aphunzitsi nd kugwexa boma???umbuli bax,mukufuna tonxe tichite kuxiwa kt xool munaxiira std…..
Zikugwirizana bwanji nfikulanda boma? Mukuoneka kuti ndinu achipani koma awa si andale ngati inu. Mukuganiza kuti aliyense angakhale wachiani chanu? Tsiku lina maganizo anuwo muzayambe mwaganiza musanapeleke mpata ku zala zanu kulemba. Mulibe umu nkhani yogwetsa boma.
Litengetseni Bomali liziwe kuti likulephera. They should not sponsor party functions to destroy their opposition yet failing to take such money to pay you-Hard workers ukwiiiii!
True! Enafe tagwira ntchito over 30 years koma salary yake so pathetic. Naji akachotsa PAYE ndiye peanuts yet kaliati and company with no qualification ma million after a month in politics. Mathanyula anyeredwe basi. Tamutopera!
It is indeed high time when our government starts showing respect to these hard-working taken-for-granted and burdened citizens. When the ‘courts-keepers’, ‘ACB’, ‘Doctors-Nurses’ demand for increments, allowances etc the are heard with the first cry they make but when it is these humble workers, they are told to go and “seek for other employments or business to get rich’. I say it is high time my friends you make yourselves felt and heard because you deserve far much better than what you are given. Stand up for what is yours!! You have sweated enough sweat and dont take it any… Read more »