Email a copy of 'Malawi to privatise hospitals, mortuaries' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

58 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
bingu
bingu
8 years ago

Agalu ose amene anavotera pita 40 pano aona

Kwaweni bolosa
Kwaweni bolosa
8 years ago

This man is a disgrace an kungofuna u president chifukwa mchimwene wake amakhala president nonsense.
Are you sure Peter of what you are saying or you are joking?
This country has failed you as a result people will stop paying taxes if you are going to predictive hospitals.
The money we could have paid taxes we will be using them to hospitals agree?
Otherwise dziko lakulakani bwana inu sa malawi mabvuto athu simukuwadziwa. Chitsiru ndi chomwe chidakuvoterani mulungu achitembelere.
Inunso mufe ngati achimwene anu.
Mwatikwana.

rich lilongwe
rich lilongwe
8 years ago

masiku omaliza ano

cj
cj
8 years ago

akanati tikugulitsa escom palibe akanadaula coz anthu amenewa amonjeza koma akamagulitsa zipatalazo akulitsenso ndi mra yomwe coz they will be no point paying tax ndalama za msonkho tizikalipila ku chipatala coz hospital bill are way too expensive

cj
cj
8 years ago

mr president are you trying to say amene anakumangilani zipatala zonsezi ndiopepela kuti inu mungobwela ndikugulitsa? Apatu mwaonetsa kuchepa kwa nzeru zanu, ndipo ngati amalawi linali tsoka pokuvotelani mulungu atikhululukile

Joseph Moyo
8 years ago

timacha ngat uchite pvtise ife watitopesa ndpo president doesnt need jet koma school leaver who are not employed must b give loan to do business of their choice pot ntchito simukuwalemba kupanda kutero2019 tizavotera tonse kape wina osat iwe ai

Joseph Moyo
8 years ago

a Malawi timadula msonkho kut azigulira mankhwala mzipatala kulipiranso ogwira ntchito ndyeno akachita privatise zipatala tizidulanso nsonkhobe?What for muganize mmene akuzunzra mmisewumu traffic kut chedwesa tikupta kukawagwirira ntchito kut atidule malipiro awo.zimandiwawa.ndpo sindkuona phindu lodulidwa msonkho komanso APM chyambireni palibe akupanga chokomera wanthu he is another diktator mmene wathesera jc ,pano zipatala koma pomaliza5yrs awononga zonse.university ed is for the rich .monga kuthesa kwa jc saziwa kut kwaononga business ya ma pvt school?Plichifukwa chanji chotumizira mwana ku school yodula chonsecho sazalemba mayeso?Azasyana chani wa jc wa cdss ndi kaphuka?Mopempha tulani panso iz sizomwe timafuna ai chonde musationongere zikoli tilibe kolowela… Read more »

Ghadhaffi
8 years ago

Mukunamizir kutukula ntcto zaumoyo kuli kulepher kwa boma lanu. Ngat mankhwala akusowa mzipatala inu ntcto yanu ncyan? Kod solution yothetser mavuto ndiyo kugulitsa zipatala? Conde che pulezidenti perekani uta ndi mpaliro kwa odziwa kuponya inu muthawitsa mbawala. Taonaninso padzana paja munavala suti,taye nga! pakhosi nkukwer mumtengo wa mango nkumadya mango tinakudzudzulaninso kt sizikukukhalani,bwanj simumva kuzudzulidwa? Bazilekani izi sizikukukhalani. Kod inu munaphunzir za ulimi wa agalu ncfkw cyan mukuloweler ku ulimi wa nsomba? Citani manyaz ndpo umunthu ukulamuleni.

josiah
josiah
8 years ago

Asilikali atenge Boma. Pitala walephela. madala zakuvuta, thula pasi undinfo galu iwe. ukagulisa zipatala ngati iwe unamangapo chako Chipatala. kagulise Ndatha farm ya ubuthi wako.

Gwatyamaru.
Gwatyamaru.
8 years ago

Mabwiya,elhapo moilephera wetiha.Mukhulhe mahiya wene.Zonapwa zyenzyo unapangewenzyo.Oroweke owaninya u Amereka.

Read previous post:
Mzuni student elected president of Malawian Midwives

Mzuzu University’s fourth year nursing student Charles Amos has been elected new country representative for the Association of Malawian Midwives,...

Close