Email a copy of 'Malawi under pressure to pass Marriage Bill' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

11 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
King salijen
King salijen
9 years ago

Zopanda mchere

Nathan Laston
Nathan Laston
9 years ago

ndibwino kuwaikila zaka zokwatirana komanso kuika lamulo lokakamiza mwana aliyense kupita kusukulu kuti malawi likhale dziko lozindikira ndi lozeka

mery julius
9 years ago

Kodi mukati 18yrs is not responsible kulowa m.banja mukufuna mutanthauze chiyani?

Molicious pwandapwanda
Molicious pwandapwanda
9 years ago

18 yrs. Ndizaka zoyenera kulowa m’banja, coz mmene moyo uno uliri 22yrs ndipatali mukungofuna podyera. Ife eni ake achinyamata tikuona kuti 18 yrs ikukwanira

Tiko
Tiko
9 years ago

Yavuta donor money. Munadya koma utsi sunatuluke. Malawi kupupuluma ndi malamulo? Lamulo loyambilira apa ndi compulsory education.

Ntchisi boy
Ntchisi boy
9 years ago

Are you trying to tell me that somebody should be free to get married if they are 8 years old simply because its their right ? People should get married when they are matured enough biologically , psychologically and even economically. Sorry to say this , but early marriages which this bill is trying to discourage are a major cause of abject poverty and high levels of dependence in our society. Unless you want Malawi to stay poor for the next 1000 years then their is some merit in your reasoning guys!

sinoya
sinoya
9 years ago

Ndipo balibe chinthu chonyasa ngati kumupangila mwina nthawi yoti adzakwatiwe,anthu amatha nsinkhu mosiyanasiya,izi zichitisa kuti uhule upite patsogolo ngati njira imozi yothesera zilakolako kwa omwe atha msinkhu.

vindere
9 years ago

Muaphwanyira ufulu a Chawa ndi Mulhako. Mitundu yiwiriyi ndiyokonda ayichukucha kwabasi. They believe in quantity and not quality. Mxiii!!!

bikoko
bikoko
9 years ago

The fact that you want to date limit adge for marriage is a significant of rights violation because its not the choice I the individual. Late the choose when to get married

Yobe boo
Yobe boo
9 years ago

Ufulu kumaulemekeze mbali zonse. Mukuwaphanyira ufulu kuwapangira zaka. Asiyeni ngati Ayawo ndi Alomwe, alibe kuwona zaka, koma kukwanitsa.

Read previous post:
Britain says visa grant rate for Malawi visitors high

The British coalition government has a painted a rosy picture on the way its Home Office  has been handling visas...

Close