Email a copy of 'Malawi woman arrested for possessing Indian hemp' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

21 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Dudu
Dudu
9 years ago

Why waste time and resources on keeping this woman in custody? Is chamba really that bad?

Dobadoba
Dobadoba
9 years ago

Kenako timva kuti amupatsa 10 year with hard labor. Koma wa Cashgate akungoyenda pa town mtima uli mmalo.

Hapuwani
9 years ago

What kind of security is this one? why not tightening the secury where these plants are grown???????? Mxiiiiiiiiii.

anduna
anduna
9 years ago

Mutayeni palibe mkhani apa osalimbana ndi nacgate bwanji?

GONAMKULAWE
GONAMKULAWE
9 years ago

SANAFUNE KUTENGA ZA NAC MUSIYENI

Nzeru Nkupanga
9 years ago

Release the poor woman and don’t charge her at all these are effects of rampant corruption at the Governments top level had it been that Big politicians and government officials managed our resources accordingly we would not be talking of people resorting to selling CHAMBA for their Families survival this is also similar to those cases involving Charcoal sellers ANTHUWATU Ndiumphawi ukuwachititsa zonsezi Ndipo vuto silamunthu ayi koma atsogoleri akatangale ngati Arthur Peter Mutharika amene akuchita promote Corruption Mumati atani Kodi nanga Pilizi akabe kenako timuwotche ana ake Akhale pa Umasiye Muziwanzunza STOP HARRASING THE POOR Timangileni achina Mphwiyo, Lutepo,… Read more »

peter mateyala
peter mateyala
9 years ago

Anakapanga bwanji mzimayi dollar yashupa pa malawi aah koma mutayeni ka mzimayi kathamange pa town, koma masambawo osagulitsatu inuyo mwatenganu.

Penu says
9 years ago

Ameneyu sanabe ndalama za boma ayi.Chambatu ndi mpamba kusiyana ndi kuba ndalama za misonkho ya anthu osaukafe.Mutayeni ameneyo Inu apolisi mangani anthu a cashgatewo

Bwetu wa kuMatanda
Bwetu wa kuMatanda
9 years ago

Mayi odzilimbikira uyu……..bola pamenepa kusiyana ndi kuchita uhule. Usadandaule mkazi akupatsa fine yochepa ndipo ukangotuluka ukanyamule katundu wochuluka kuti uzabweze makobili ako. Anthu odana ndi chilungamo awa,……, akufuna uzichita kudyetsa katundu kuti upate? Shupit!

Mwananyasa
Mwananyasa
9 years ago

Abale, stop victimising people ndi Nkhani ya chamba. ikani lamulo lokomera onse including government on this issue. It is not right for the government to be harvesting Chamba on the roads through A polisi. Tandiuzani, ndi liti lomwe Boma linaotcha or publicly destroy all the tonnes and tonnes of chamba chomwe mwakhala mukumatiuza kuti mwalanda anthu? liti? so where is it all? where is the warehouse? it must be a BIG one! and who is paying rent for it? ndiye chambacho! asiyeni anthuwa or regularise the trade and consumption means.

Read previous post:
Celebrating St Andrew’s Day in Scotland’s special year

This year, we have been marking 50 years of Malawi’s independence. Malawi’s history has a strong connection with the UK,...

Close