Email a copy of 'Malawian man arrested for selling ‘dog meat’' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawian man arrested for selling ‘dog meat’' to a friend
Malawi Police Service have justified the arrest of late Tasokwa Msiska's children and cleared Minister of Information, Jappie Mhango of...
too much mphakana kugulitsa galu ngati nyama? Ameneyo alangidwe kuti anthu amene ali ndi maganizo amenewo atengelepn phunziro
kkkkk. Balaka again
Masiku omaliza chikondi chizazilala,chimenecho ndi nkuluyu mpaka nyama galu apa ndiye mwaonjeza man,nanu anthu kumangodya zili zonse.
Ndiye mumumange?? Sakukumvetsani chisoni ameneyo??? Mumuleke,,anthu amadya amphaka,,agalu,nkhumba..zimasiyana chani??? Vuto ndi anthu ankhwiluwo.akafuna zabwino akagule ku cold storage.,.iya
life bigginz with eating meat dog
Olo mwala anthu akudya bola kuukazingila bwino
Mmmmmm God help us
kodi ndi angati adwalapo atadya nyamayo? Musiyeni munthuyo bola anthu adziwa kuti mkuluyo amagulitsa galu
Breach of peace, when actually it brought peace after kukhuta. Wasowa mlandu apa, mtsyeni basi. Revise our laws to be relevant to certain cases
Anthu amadya FISI Ndiye mukati GALU,chiweto.Bleach of peace? Apa Ndiye sizikuigwirizana ndi nkhaniyi.Bolani adakati malonda oletsedwa.Komanso chinyengo pa malonda mmalawi muno chafikapo.