Email a copy of 'Malawians heading back to South Africa were being trafficked' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

76 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Joseph Jim
Joseph Jim
8 years ago

Welcom 2ur original home malawi land of peace just welcom this situation kukakhala bata u wil go,provided u stil alive.

Jonathan j.j.
Jonathan j.j.
8 years ago

Kodi chinthu chimene chapha anthu ambili ndiichiti, Zenofobiya kapena Aids? Bwanji anthu sakusintha khalidwe[kusaiopa] Aids yo? Ndiye asebwelele ku moyo wantofotofo ngakhale kuli zowophya? Ndiye wina wake asamanamize anthu atakhuta tiakachaso taketo kumanena kuti azaphunzitsa/kulemba anthu ntchito. Adzaapatsa ndalama zingati pamwezi zoti mpaka kugula malata zidina ndikumanga nyumba? Abale inu koma amalawi ena kuzipopa. KuJoni kwatukula miyoyo ya amalawi ambili. Anthu ambili asiya kugona munyumba zamaudzu. Tulo tabwino chifukwa cha Joni imene. Kodi anthu amene afa ndi chivomelezi ku Nepal ndi Zenifobiya imeneyo? Olo ukafuna uchi wokoma, umalumidwabe ndi njuchi. Aliyense ayandele yake. Nthawi yikakwana Yakwanabasi.

Skill amos
Skill amos
8 years ago

Sazaonekanso munthu yemwe angakwanise ku bwenzelesa dziko mmalo mwake chifukwa kunalembedwa kale tsono dzikuchitikaz nzongo kwanilitsa malembo,abale ndi alongo chonde ndimveseni ndimveseni inosinthawi yolimbana ndikulozana zala ayi koma ndinthawi yozikonzesela moyo wanu mlaliki akut zones nzachabe ndizinthu zongosausa mtima.:(:/;(odala iye amene amve mawuwa ndikuwa gwiritsa ntchito mtendele ndimadaliso zikhale kwa iye :>:DMULUNGU AKHALENANU(filimon Amos wa mtukula)

Blessings
Blessings
8 years ago

Kulibwino kupita ku s.a. Kusiyana ndikumagula ndege yoti wina azinjoya kuchoka ku misonkho yake nkumasauka shit!

Paudala
Paudala
8 years ago

Guys Zigianizileni Anzanu Tikufewa Konkuno Ku Malawi

akilen
8 years ago

Malawi government is too corrupt and biased.It only employs their sons and relatives thats why we accept to die in South Africa.

inzo
inzo
8 years ago

U

Wachikond
Wachikond
8 years ago

Asiyeni apite aliyense ali ndi imfa yake, ena sakafa than kuti tinene kuti tiwasamala koma osakwaniritsa. Pamalawi kuti umgaire mzako chinthu ndekuti pafa mzungu. Let them go.

nyasa boy
nyasa boy
8 years ago

Malawi government must agree that we suffering to the world

Mark Markc
8 years ago

Akalawa voloso sakusika!

Read previous post:
Mzuzu University in TNM ‘smart data’ social weekend blitz

After the success of its social weekends at the Polytechnic, TNM Smart Data invades Mzuzu University (MZUNI) for Social Weekend for...

Close