kodi anayambitsa zomati ‘wamkaka’ zi ndani? A Malawi kutengeka basi aliyense timwa wamkaka… umphawiwu siwabwinodi! ine zimandinyansa bwanji!
Oikonda Bullets
9 years ago
Wishing them all the best.
yazula
9 years ago
Bhunyufu! wakutumayo akuphweteketsa wamva chamba eti,ufune usafune Big Bullets iwinabe basi ngati sukumvetsa udzilume pa mkolokolo pakopo SHUPIT!!!!!! Mxiiiiiiii
Dr. Vxorexalho
9 years ago
zabwino zonse the pples team…
Kika Kanawe
9 years ago
My plea to BB supporters to keep on supporting the team financially through the bank account and SMS Initiative.Let’s put the team in prayers the best is yet to come for the peoples team.The government and the corperate should sponsor the team.
TK
9 years ago
a Malawi mpaka Ku Sudan kkkkkkkk
osman usu justin
9 years ago
Kumamvetsa aMalawi okhala ku sudan osat masapota abullets kkkkkk
Lackson Mustafa
9 years ago
Wishing Bullets FC all the best in Sudan.I beg all Bullets FC Supporters to continue sending messages to BB 2015 through. TNM network in order for the team financially supported
Adam christon Masamba
9 years ago
Ndiri ndichikhulupiliro chonse kuti team yathu yokondedwa ya Big Bullets ichita bwino nditu. Ndamumva wina wake amene ali ndi mtima oipa osaifunila mafuno abwino team yathu, kaya sindikuntha kudziwa kuti mtima wake ndiwotani. E,e si fombon imeneyo ndi Al hilal kungobadwa ndi mtima wausatana basi, osafunira azanu mafuno abwino pamene akuchita bwino tizaonana.
zangovuta kugnja neba
kodi anayambitsa zomati ‘wamkaka’ zi ndani? A Malawi kutengeka basi aliyense timwa wamkaka… umphawiwu siwabwinodi! ine zimandinyansa bwanji!
Wishing them all the best.
Bhunyufu! wakutumayo akuphweteketsa wamva chamba eti,ufune usafune Big Bullets iwinabe basi ngati sukumvetsa udzilume pa mkolokolo pakopo SHUPIT!!!!!! Mxiiiiiiii
zabwino zonse the pples team…
My plea to BB supporters to keep on supporting the team financially through the bank account and SMS Initiative.Let’s put the team in prayers the best is yet to come for the peoples team.The government and the corperate should sponsor the team.
a Malawi mpaka Ku Sudan kkkkkkkk
Kumamvetsa aMalawi okhala ku sudan osat masapota abullets kkkkkk
Wishing Bullets FC all the best in Sudan.I beg all Bullets FC Supporters to continue sending messages to BB 2015 through. TNM network in order for the team financially supported
Ndiri ndichikhulupiliro chonse kuti team yathu yokondedwa ya Big Bullets ichita bwino nditu. Ndamumva wina wake amene ali ndi mtima oipa osaifunila mafuno abwino team yathu, kaya sindikuntha kudziwa kuti mtima wake ndiwotani. E,e si fombon imeneyo ndi Al hilal kungobadwa ndi mtima wausatana basi, osafunira azanu mafuno abwino pamene akuchita bwino tizaonana.