Email a copy of 'Martha Mwangonde is new Ombudsman : Malawi public protector approved by Parliament' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

45 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
KK
KK
8 years ago

Koma abale zawonekelatu kuti Atumbuka mitu yawo siyimagwila . This woman is not a Tumbuka but she is carrying a mbwenu mbwenu surname because of marriage. Ndimanyazi omwe alibe amvekere wakwithu, wakusambila Koma ku, Malawi dziliko.

allenanjanji
allenanjanji
8 years ago

By the way Pepani anzathu atumbuka Martha is not a tumbuka she is from Nkula! Congrates my dear classmate at
Zingwangwa Secondary School, thats coming! Go! Go! Go! Zingwangwa! Munya muona atumbuka! Kalemba woyeee! Martha woyee!

tuntyufe
tuntyufe
8 years ago

congrats Martha. YARO 97 is doing really fine you have made us proud!

kate
kate
8 years ago

Congrats mwana wakukaya. koma Atumbuka mukubwera boooo. School inatikhandiza mweeeeee. We will remain ever shinning. Tawonani mpaka Peter kuganiza zokatenga Mchewa mzake kapena Mchawa at position 3 Fiona Kalemba, kuwopa kuvomera a Mr mkandawire who came 1st position kuli kuwopa atumbuka kuchita dominate all big positions? Koma yaaaa! Anyway Congrats Mai Mwangonde you came the outstanding performance on the interview and you came shinning at no 1. Pofunika kusinthadi ndi poti Mai Mwangonde should be called OMBUDSWOMAN NOT OMBUDSMAN! Zili ngati kunena kuti ‘traffickman wa mkazi’ kkkkkkkkkkkkk

Nabanda
Nabanda
8 years ago

Ndasangalala pomusankha Martha kukhala pampandowu. Chifukwa mwinano atsikana owonano ubwino wa sukulu.

kei khembo
kei khembo
8 years ago

Ai zilibwina apa mau aja oti ndife atsongoleli amawa athera ulewanu martha jerasi siumuna.

Observer
Observer
8 years ago

Enock chibwana is seen as the best because he communicated with Malawians what he was doing. He was available to the Press.

Free advice Martha! be open to the press and let them know your strategy! quick wins and long term achievements!

If you don’t have a Communications Specialist please create that post immediately.

Dusty
Dusty
8 years ago

Dziko likachuluka mabulutu mavuto ake ndilikulozana zala even people who are learned starting behaving same way as their fellow brothers or sisters.Tribalism ya chuluka chifukwa cha ubulutu,umbuli.

GRM
GRM
8 years ago

I have shared this story with my daughter Martha. This Mrs Mwangonde is a role model. Mwana wamkazi azitero. I WISH HER ALL THE BEST. Go and impress like Enock Chibwana.

waseme
8 years ago

To hero atumbuka this, atumbuka that. Kodi a Malawi tizasiya liti kukumbana mitundi? Zosankhana mitundu ndi zomwe zina zunzitsa anzathu aku Rwanda. Do u want this to happen in Malawi? mundiyankhe inu atsankhonu.

Read previous post:
MCP protest secondary school fees hike, refuse to ask minister questions

Opposition Malawi Congress Party (MCP) legislators on Tuesday vehemently protested government decision to raise fees in secondary schools, saying this...

Close