Email a copy of 'MCP fires seven District Chairmen over dissent' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'MCP fires seven District Chairmen over dissent' to a friend
Tempered flared in the High Court Wednesday morning in the trial of attempted murder of former budget director Paul Mphwiyo...
SURELY ALL THESE R FROM DPP
Dpp causing all the confusion. Go deeper you will find that the confusionists have been paid by dpp thugs.
Yes Analyst, dpp is smiling.
y cnt u liv DPP alone,zawo zikuyenda and u r bzy, talking a bt them, mk ur party strong nanga akayamba kukukwenyani za cashgate money fr campaign given by JB ,muntha ngati pp,ma members adzituluka every hr
Zingayambe kuyiwalika muli ndi mnthawi ya kamuzu mkuti muli a youth bwenzi pano muli ku shire river ng’ona zitakudyani, inu simukuona kuti menyani khalidwe lake ndi lang’onali, zikuoneka achakwera siyatha kukhala ndi ana, kukhala ndi ana ndikuwatong’orera pang’onopang’ono zonse mukungokudya nokha amatelo ana mkumawa opyseza si mwaona mumasekerera pp koma pp imaononga chipani inu osadziwa nanga ngati imapanga zimenezi pp yokha mukhale pansi muonanso kumkati mwanumo mulinso a dpp amene amalandila salary kuchokera kwa ku dpp koma simudziwa modzi waiwo ndi uyu waku……. Koma amene mukulimbana nawo achimenya ndiye mcp yeniyeni imene sisintha mawanga olo pangono koma inu pompano tivakuti… Read more »
Mwayamba chibwana 7 ???
Long said MCP is lacking matured politicians who csn lead the party. The party works on assumptions which are dangerous. Position holders of yhe party are not real poliyicians as they have shown that thry are not avcomodative. Issues raised by senior party officials taken setiously would propel the party but chose to down play them. Be rminded trusting the so called polical analysts of Malawi wouldnt assist cause i see them despite being educated they lack analytical ecumen. How many times have goofed ? Thdy hzve appeasement policy and mcp think csn sway the prople. This is yhe time… Read more »
Amalawi ndinu dziyanthu dzopusa, I don’t understand why u always hate (DR.CHAKWERA) So the people who been fired, they wanted to destroy MCP, if you find out you will see that , DPP is behind those who just fired, But Chakwera.
Amalawi ndinu dzitsilu, simumadziwa chimene mumafuna Pamoyo Panu, Chimene mukulimbana ndi DR.Chakwera ine sindikuchiona, amalawi munazolowera kuvotela Mbava; Those People they need to destroy MCP, that’s why MCP fired them before its too late, if you can find out” you can see that DPP is behind those people, Dzuka Malawi!
plz mr chakwera izi zikuipitsirani mbiri zituleni pansi.tiziti adpp ndi omwe akuwatuma ma district chairman? pajatu amnzanu a pp zikawasokonekera dey blame dpp. all oppositon parties they can’t win in 2019.malo molimbikitsa zipani zanu ur bzy kukangana so do u think u can win.Weak minded leaders hv no future & its e.g mcp learship no future at all plz obaba come back 2rescue mcp cz zikuchitikazi chipanichi chikutha. w need experienced leaders not chakwera or kabwira they’re immature whr z njovuyalema de likes of jumbe imean dis mcp mmmm they can’t stand cme 2019
Tiye konko waziyamba dala