Email a copy of '‘Miracle money’ lures Malawi artists into gospel, working with Prophet Bushiri- Report' to a friend
Loading ...
Email a copy of '‘Miracle money’ lures Malawi artists into gospel, working with Prophet Bushiri- Report' to a friend
For many Malawians that I know, the freedom to criticize the government of their country is not inspired by some...
KODI ANTHU A MULUNGU N DIKUFUNSENI,KODI MUMADZIWA BWANJI KUTI PROPHET BUSHIRI NDI WA SATANIC?KODI MUMADZIWA BWANJI KUTI MACHILITSO AWA NDI A MULUNGU AWA NDI A SATANA? KODI MULUNGU MUDZAMUKHULUPILIRA LITI KUTI NDIOLEMERA?KODI BIBLE MUMAWELENGA INU? KODI MAU OMWE ANANENA AMBUYE YESU AKUTI MUNTHU YEMWE ADZAPANGE ZOFUNA ZA MULUNGU ADZAPATSA MPHAMVU NDIPO ADZAPANGA ZINTHU ZAZIKULU ZOPOSA MOMWE CHRISTU ADACHITA ALIPA DZIKO LAPANSI LINO? CHONDE ABALE NDI ALONGO MUSADZICHEDWETSE NDIKUPANGA DZAWENA NANUNSO TAPEMPHERANI MOLIMBIKA MULUNGU ADZAKUPATSANI ZANU KOMA MUKAMALIMBANA NDI ANTHU OMWE CHAUTA WAWADALITSA NDE MUMADZIPANGITSA KUTI MULUNGU ASAKUKHULUPILIRENI COZ INUYO SIMUMAKHULUPILIRA KUTI MULUNGU NDIYE MWENI CHUMA.
Mr Daniel Theu? Be aware! Open your eyes and see.. This is the world full of dirty games. Devil has powers to heal the sick, feed the needy and anything u can mention! Remember that we are living in the last days!!!!!!
Zochitika masiku omaliza, anthu azakonda ndalama
Victor, you wrote your thoughts all about the prophet. I am only asking you to attend to the prophet’s meetings and understand him well. You can even watch the prophet channel on your dstv or go to “you tube” pages of him before critics. I hope you have never come across a man like him in life and ask yourself, why now? He is feeding the needy from southern region to northern region of Malawi. He is praying for the sick and people get healed instantly, he is teaching people good news not only in your country but the whole… Read more »
Miracle Money? ReallY? You mean we should we be sitting idle waiting for miracle money–money to come in our pockets just like that? Why then does the Bible say that he who does not work should not eat? What I know and believe is believers operate in financial prosperity via the Law of Seed Time and Harvest. God says in Genesis 8:22 that “While the earth remaineth, seed time and harvest, and cold and heat, and summer and winter, and day and night shall not cease.” This entails that if you are to prosper financially you must be willing and… Read more »
Tidzawona pa siku lomaliza Lipenga likadzalira!
Jesus is a brand that has been sold to many people since they were in nappies, so anything no matter how trashy the music can be as long as it has jesus in it, you are going to sell to people infected with the religion virus of the mind. Marketing people know this very well and they know it will work.
Nanga magospel singes are u leaving to expectations?Thocco mbiri yako yanunkha kuno?wathesa banja la zimatha.mai wamvano kumupanilila osaopa kuti sisayizi yako !amako amene aja kungoti amaoneka chisikana chifukwa ndi chumba!zoona wasintha nyengo yake!
A Thocco Siyani gospel mukutichitisa manyazi.Banja wathesa la anthu akuluakulu !mai wamvano kumudyera ndalama zake !
Koma bola osathesa maukwati a anzanu magospel singers inu.TK ndi uja wathesa ukwati wa GSP !Koma iweyo osaopa ayi?ndimayesa amene uja ndi mako mpaka kumupanilila !mai wamvano kumulakwisa kkkkkkkk zoona wasintha moyo wake!munthu anali pa chinyezi lero ali padwale !amayemda pa ma prado ,rover ,hilux koma lero akukwera kabanza !Zoona TK wasintha moyo wa mayiyo !oops paja ndi chumba ndiye umayesa saizi yako ee a gospel singer!