Email a copy of 'Mother gang up with son to kill hubby: Malawi Police arrest her, son on the run' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Mother gang up with son to kill hubby: Malawi Police arrest her, son on the run' to a friend
The International Women’s Association of Malawi (IWAM) has pledged to continue working hand in hand with Beautify Malawi Trust (BEAM)...
kkkkkkkkk! This is man slaughter not murder. muwapatse bello
So the father was 16,the mother 9 when the run away son was born?Sounds unrealistic!
Should be step son to the mother
Olemba nkhani kunama ngati muna chita kuchekela anabeleka Ali ndi dzaka 9 nachengwa
wandilaula
Hahaha! ndiye mwa amayi 25 mwana 16? Ok tiyeni tipange kaye masamu apa: 25-16 = ?
25-16 = 9
Ndiye amayiwo anabeleka ndi zaka 9? koma abambo anali ndi zaka 45?
Ok tipange kaye masamu apa:
45-9 = ?
45-9 =36
Hahaha abambowo anagwirilira mwana wa zaka 9 pamene iwo anali ndi 36!
Anyway RIP!
If she gave birth at 9 then she’s had a tough life and life turned her into a savage. Si nanga amuna aMalawi mumakonda kubereka ana osawasamalanso?
Why is the boy called Maliro when the parents are Chinangwas? Maybe the boy felt the father was not his so the murder.
Amai anchiuno awa anabereka Mwana Ali ndi zaka 9?
my point really……. giving birth at 9? zosatheka unless ngati ali mwana wa a bambowo wakunjira
Amai ndi abambo akusiyana 20yrs
size kukana
KUSUSUKA NDI GAIWA ANGULUFE
SICHINA