Email a copy of 'MP queries arrest of Msiska's children over Jappie funeral saga' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'MP queries arrest of Msiska's children over Jappie funeral saga' to a friend
Heavy rains accompanied by high speed wind have blown off house roofs in Blantyre and damaged some vehicles as the...
japie let me warn you, why are u illtreating people from your motherland.you are cruising dangerously ,and you are about to fall
stupid mbwenu mbwenu.if you are inteligence why malawi has never been led by stupid mbwenu mbwenu since independence?
SURELY, CHEAP MPS DO NOT LAST MORE THAN FIVE YEARS IN PARLIAMENT ESPECIALLY IN THE CONSTITUENCY WHERE HONURABLE JAPPIE MHANGO COMES FROM.THAT PART OF MALAWI IS ONE OF THE CONSTITUENCIES WHERE LITERACY LEVELS ARE VERY HIGH. I FEEL SORRY FOR JAPPIE MHANGO FOR BEHAVING AS IF HE COMES FROM SOMEWHERE IN MULANJE OR THYOLO. ONE PARLIAMENTARY TERM WILL BE ENOUGH FOR HIM!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!
Who is Jspiemhangi kape wodyanawo. Kafunseni a ksmlepo ksluws or chihans ndsle ximakhala bwanji…
Mafumu akuononga midzu ndi anthu ndiye ngsti rnsnu mudachoka ps khomo pa mfumu zanuxo,enafe tidachoka pankjoma pa mai anthu nkuyiyumuza ke xul mpaka college…. Mfumu has no ingluence what i fo only the laws of the land..inshoty want to ser prodperiyy hsrmony and redprct of all vitizens rihhts!
CHIHENI AKUTI ULI SONO?
CITIZEN
I have never seen stupid people like you, my fellow northerners open up your eyes and don’t be used just as a condom. Don’t you see that the mcp wants to just use you in 2019? Issues coming out at a funeral are dealt at a funeral, why taking it to parliament ? Is parliament a place of kuthana than discussing real issues affecting Malawians? We are not stupid, we are following the deliberations and shall see!
This issue is important to be well clarified.because its like he is using his political powers to downpress others.on the the hand let us also be frank it is not in parliament where the follow up to this story should be taken
OLEMEKEZEKA ANDUNA!unduna sionyadira salowera mkalasi.you are spoiling ur political milage by abusing your office.mukuphwanyaso ufulu watolankhani.Nanuso osankha nduna.mumaonachani posankha?azingoipitsa mbiri yanu ndiya dpp yonunkha kalei!
Tinene muchinenero chathu chonde inu aboma kapena ochuluka mphamvu, nkhaniyi kumaliro siiyanu a Police.Ukutu ndi kumudzi ndipo kuli otilamulira mafumu amene wina aliyense kaya ndi nduna, pulezidenti,mp,msilikali,ndinso maudindo osiyanasiyana tonsefe timachokera mnyumba zawo mafumuwo.Apapa aFumu ndi amene akanaweruza ana awo kuunika zimene zinalakwika.Sipachipani, kapena msonkhano wa boma ndipo ndizokhuzana ndi boma koma zapamudzi ndipo eni wake ndi aFumuwo ndi anamfedwa iwe Jappi walowerera ndipo ukuderera mafumu kumudziko? Wayiwala ntchito yimatha chibale sichitha.Maudindowo mukapasidwa chonde simuzaafa nawo ndipo ma examples muli nawo ndithu taonani John Tembo,Muluzi,Kachale,Joyce,Malewezi,Kadzamila etc.Ndizosiyirana zinthuzi anthu wamba awa apatseni ulemu mawa ndi anzanu omwewo.Ndipo kuchita kukhala ngati temberero… Read more »
Good Samaritan, what we want is justice, the perpetrators of violence in both cases should be taken to book