ACB and judges get thd points here raised by patriotic Malawians,MANYUMBAWO ALANDIDWE APO BII FIREGATE ISAWAPITILIRE AMENEWA
S Allie
9 years ago
Let’s wait and see for the court to do the job if not malawian will remain be poor forever
OBAMA
9 years ago
Even mu area 47 kuona nyumba mwini wake ndi driver wa boma ku ministry yinayake koma ali ndi nyumba mu area 10 and 47. Ndalama anazitenga kuti amenewa. Cashgate basi with this beauracratic system of government we have causes people to steal money in the government. Amene akukana zotseka account number 1 ndi amene akufuna kuti aziba ndalama za boma and one of them is Atupele Muluzi. Pa debate paja ankakana za maganizo otseka account number 1.
mr man
9 years ago
yes mrs senzani ali ndi nyumba pa bunda ,kuiona nyumbayo its close to 1 billion kodi ndalamazo azitenga kuti .iwe mphwiyo umati ndiwe odalitsika mchifukwa uli ndi ndalama zambiri tikulanda nyumbayo, mabillion ambiri amenewo ,inu a ac b mukalephela ndikhalapo ndine kuti ndithane nazo
ezy u. k nbimenya nkhondo
chris Nyirenda
9 years ago
INU ACB NANGA TINAWELENGA KUTI PETER D MLAUZI ANACHITA CASH CHEQUE CHA TWENTY MILLION KWACHA NKHANIYI TINAYIWELENGA PA JANIARY 5 CHAKA CHINO KOMA MPAKA LELO AKUTI NDALAMAZO ANAGAWANA NDI AMENE ANALI REGISTRAR WA HIGH COURT MLAUZI NDI DEPUTY SHERIFF OFF MALAWI WOLANDA KATUNDU WA ANTHU OSALIPILA NGONGOLE ACB WELL DONE FEAR NOBODY
lehlonolo majoro
9 years ago
you stupid fools rush to arrest people without knowing what they did wrong???? acb my foot, mbaza zeni zeni!!!!!!!!!!!!!
ali tiye nazo mkaziwanga ndalama za a malawizi. nde muzawagamulenso 3 years tiyamba kuotcha nyumba za ma judgetu tikatopa nanu
Venezuela
9 years ago
Fufuzani makamaka ma civil servants omwe amanga nyumba zowopsyeza, amazitenga kuti ndalama like theresa senzanis mansion pa bunda. Zilandidwe zimenezi kapena apo bii kukoleza moto basi tiluze tonse. Naye mphwiyo that house, anamangila ndalama zake ziti?
ACB and judges get thd points here raised by patriotic Malawians,MANYUMBAWO ALANDIDWE APO BII FIREGATE ISAWAPITILIRE AMENEWA
Let’s wait and see for the court to do the job if not malawian will remain be poor forever
Even mu area 47 kuona nyumba mwini wake ndi driver wa boma ku ministry yinayake koma ali ndi nyumba mu area 10 and 47. Ndalama anazitenga kuti amenewa. Cashgate basi with this beauracratic system of government we have causes people to steal money in the government. Amene akukana zotseka account number 1 ndi amene akufuna kuti aziba ndalama za boma and one of them is Atupele Muluzi. Pa debate paja ankakana za maganizo otseka account number 1.
yes mrs senzani ali ndi nyumba pa bunda ,kuiona nyumbayo its close to 1 billion kodi ndalamazo azitenga kuti .iwe mphwiyo umati ndiwe odalitsika mchifukwa uli ndi ndalama zambiri tikulanda nyumbayo, mabillion ambiri amenewo ,inu a ac b mukalephela ndikhalapo ndine kuti ndithane nazo
ezy u. k nbimenya nkhondo
INU ACB NANGA TINAWELENGA KUTI PETER D MLAUZI ANACHITA CASH CHEQUE CHA TWENTY MILLION KWACHA NKHANIYI TINAYIWELENGA PA JANIARY 5 CHAKA CHINO KOMA MPAKA LELO AKUTI NDALAMAZO ANAGAWANA NDI AMENE ANALI REGISTRAR WA HIGH COURT MLAUZI NDI DEPUTY SHERIFF OFF MALAWI WOLANDA KATUNDU WA ANTHU OSALIPILA NGONGOLE ACB WELL DONE FEAR NOBODY
you stupid fools rush to arrest people without knowing what they did wrong???? acb my foot, mbaza zeni zeni!!!!!!!!!!!!!
ali tiye nazo mkaziwanga ndalama za a malawizi. nde muzawagamulenso 3 years tiyamba kuotcha nyumba za ma judgetu tikatopa nanu
Fufuzani makamaka ma civil servants omwe amanga nyumba zowopsyeza, amazitenga kuti ndalama like theresa senzanis mansion pa bunda. Zilandidwe zimenezi kapena apo bii kukoleza moto basi tiluze tonse. Naye mphwiyo that house, anamangila ndalama zake ziti?
kenaka muwalipire ndalama chonsecho mukuchedwesera dala.