Email a copy of 'Mr. President, more kisses please! Malawi First Couple' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

46 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Kondwani bwande
9 years ago

Vuto apa palibe. Anakisa azikazi anu. Ndinthawi yake

apo
apo
9 years ago

pali nkhani apa? anthu asa kisane…. vuto ndi chani? kisanani poyera ma hope a freeze kumene……inu koma zogololo ndi akazi aeni mxiiiiii

john
9 years ago

kiss imakolezera chikondi inde koma kiss yamalovu pagulu siyabwino or pangono bola yapa tsaya osati mpaka lilime mkamwa aaaà president?? its private love.

Dedza
9 years ago

Yes very nice

Malawi
Malawi
9 years ago

They are not commiting sin. They are lawfully married and there is nothing obscene. Whats wrong with people? Some of u who are against this love act ndi ma jelasi basi. You have never kissed ur wives koma mahule. Leave APM andhis lawgully wedded wife alone.

johnmandeule
johnmandeule
9 years ago

Mr. President ndiye kufewa kumeneko

victoria Dim
victoria Dim
9 years ago

Me like

Noxiebj
Noxiebj
9 years ago

Kaya bolani ali pa banja…. Za kiss zo ine ndie log out…kkk

CHILOMBO MPSYALA
9 years ago

Anthu odya maliro sayamikira aliyense ngakhale atachita bwino bwanji.APM ngakhale akasanduka mngelo mkumakwera kumwamba ngati ELIYA wa mBaibulo Anthu bwezi akuti walakwa President sapita Kumwamba .Anthu ozolowera kudya matewera wobibirawa sitingawadabwe.

phiri la dzunje
phiri la dzunje
9 years ago

Nkhani yake ndiye iti pamenepa mwasowa zolemba eti president analakwa chiyani mkaziyo ndi wake ambilinu mudachitira umboni ukwati wao ndiye pa valentine asapatse kiss kwa okondedwa wao walakwa president pagulu pagulu ndiye kuti chiyani.Asanakwatile ndinu nomwe mudampatsa maina ambili mbili lero ali ndi mkazi bwanji akupeleka kiss pa gulu a malawi sitidzathekanso ndife dzitsilu dza wanthu mbuzi za mano kusi godemeti

Read previous post:
Prophet Bushiri appointed president of AFRICCI: Secures money for African developments

Leader and founder of the Enlightened Christian Gathering prophet Shepherd Bushiri has been named president of African Christian Coalition for...

Close