Email a copy of 'Muluzi tasks Malawi Muslims to embrace peaceful coexistrence' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Muluzi tasks Malawi Muslims to embrace peaceful coexistrence' to a friend
Lilongwe based golfer Frank Mvalo earned himself bragging rights when he won this year’s Nico Life Invitational Golf tournament played...
Kunena zoona amalawi sitizapeza president ngati Bakili Muluzi munthu wachikondi wantendre wodziwa mavuto mudziko kwa ena kwao kuba basi sadziwa mavuto
AMALAWI IWALANI zozapeza PRESIDENT wina ofanana ndi MULUZI ngakhale mutamenyesa nkhwangwa pamwala Iwalani
Koma nkhani yontukwanila Muluzi nde iti?.Yomwe yolangiza his fellow Muslims -yi?.
SIBWINO.
Jelasi basi a Malawi
Let us preach peace as indicated above. Bwanji mtopola inu. Akuonani mulungu tu
Siyanitsani moyo wa inu ndi President wopuma osatitu kupuma pa khasu,iye komwe angapite atolankhani amakhala akutsatira ndiye mumafuna akane kumutenga zithunzi inu nomwe mukanapanga react bwanji osamangolankhulatu chifukwa choti basi anakupatsani pajama, kumalankhula mukugwiritsa ntchito mzeru please. Ngakhale zikunyaseni ku Malawi sikudzapezekanso mtsogoleri ngati Tcheya.
In response to Mhesha comment # 16. We all go to our home villages we just don’t publicize our visit like some stupid politicians. i wish someone would tell these dunderheads how stupid they look.
nsapatozo anamupatsa nd saulosi during public service reform….nza DPP
@ WIN . B
UNANGOBADWA OPANDA MANYADZI MBALE. MALEMU BAMBO AKO PEPANI KAYA NGATI ALIPO , NSAPATO DZIMENE DZIRI NDI ATCHEYA SAKANAKWANITSA KUGULA OLO AKANAKALA KUTI AGWIRA DZAKA 40.
NGATI AMALEPERA KUGULA KABUDULA WAMKATI OLONGOTSOKA NDIYE NANJI SAPATO
IWE UNDISAMALETU !!!!!!!!
Atcheya is only blue in shoes but the rest is yellow.Look at his yellow chairs.Ka schooner ndikamene kali blue.Mwausinjatu kuchitekete.
Atcheya ka nsapato ka blueish konkera kwa chizimayi mwandiwaza nako.Kalibwinotu kameneko achalulungwa.