Email a copy of 'Muluzi tasks Malawi Muslims to embrace peaceful coexistrence' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

29 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Dennis
8 years ago

Kunena zoona amalawi sitizapeza president ngati Bakili Muluzi munthu wachikondi wantendre wodziwa mavuto mudziko kwa ena kwao kuba basi sadziwa mavuto

ibrahim makwati
ibrahim makwati
8 years ago

AMALAWI IWALANI zozapeza PRESIDENT wina ofanana ndi MULUZI ngakhale mutamenyesa nkhwangwa pamwala Iwalani

Ishmael Makwinja
Ishmael Makwinja
8 years ago

Koma nkhani yontukwanila Muluzi nde iti?.Yomwe yolangiza his fellow Muslims -yi?.
SIBWINO.

omar khaliffa
omar khaliffa
8 years ago

Jelasi basi a Malawi

ochewa
ochewa
8 years ago

Let us preach peace as indicated above. Bwanji mtopola inu. Akuonani mulungu tu

SHAMS HASEEB
8 years ago

Siyanitsani moyo wa inu ndi President wopuma osatitu kupuma pa khasu,iye komwe angapite atolankhani amakhala akutsatira ndiye mumafuna akane kumutenga zithunzi inu nomwe mukanapanga react bwanji osamangolankhulatu chifukwa choti basi anakupatsani pajama, kumalankhula mukugwiritsa ntchito mzeru please. Ngakhale zikunyaseni ku Malawi sikudzapezekanso mtsogoleri ngati Tcheya.

Ntakataka
Ntakataka
8 years ago

In response to Mhesha comment # 16. We all go to our home villages we just don’t publicize our visit like some stupid politicians. i wish someone would tell these dunderheads how stupid they look.

WIN.B
WIN.B
8 years ago

nsapatozo anamupatsa nd saulosi during public service reform….nza DPP

SHAKA
SHAKA
8 years ago
Reply to  WIN.B

@ WIN . B

UNANGOBADWA OPANDA MANYADZI MBALE. MALEMU BAMBO AKO PEPANI KAYA NGATI ALIPO , NSAPATO DZIMENE DZIRI NDI ATCHEYA SAKANAKWANITSA KUGULA OLO AKANAKALA KUTI AGWIRA DZAKA 40.
NGATI AMALEPERA KUGULA KABUDULA WAMKATI OLONGOTSOKA NDIYE NANJI SAPATO
IWE UNDISAMALETU !!!!!!!!

Mavalidwe
Mavalidwe
8 years ago

Atcheya is only blue in shoes but the rest is yellow.Look at his yellow chairs.Ka schooner ndikamene kali blue.Mwausinjatu kuchitekete.

Fashionista
Fashionista
8 years ago

Atcheya ka nsapato ka blueish konkera kwa chizimayi mwandiwaza nako.Kalibwinotu kameneko achalulungwa.

Read previous post:
Nico Life golf: Mvalo earns himself bragging rights

Lilongwe based golfer Frank Mvalo earned himself bragging rights when he won this year’s Nico Life Invitational Golf tournament played...

Close