Email a copy of 'Mutharika must not demand from Malawians what his govt won’t do' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Mutharika must not demand from Malawians what his govt won’t do' to a friend
The Centre for Human Rights and Rehabilitation (CHRR) has welcomed the conviction and sentencing of a former junior civil servant...
Abale, one solution to winning aid back is: SPEED UP THE CONVICTION of CASHGATE and any other thefts by civil servant.
Mukunya abale anga simunati kaya ndinu a die hard a DPP kaya chani, tukwanani apa mmene munga thela, tikumane pokagula Michele pa okalapo, mtengo ndi umodzi basi. Ameneyo mukuti APM sakupelekelani Koma nokha, ndiye talalatani apa muonetse kupusa kwanu anthuwa akudziwe, pano mupeleke tax wambili kuti ma ministala agulile ma benz! lchi ndi chomwe chitakuwaweni inu mukukuntha fumbi mutayenda wapansi from area 23 to city centre!
Chilungamu n’choti azungu sakondwera ndi boma lopenya. Amafuna tidzilamulidwa ndi mabulutu kuti adzitha kutibera bwino fodya, thonje, tea, zakumigodi, mafuta etc. Azingosinthasintha mfundo muona
Mbuli chomwe mmadziwa ndikunyoza monga anthu olephera. Anyway nde mpaka zaka kuti anuwo azalepherenso.ife timalipila nsonkho sitiona chachilendo
yes
malawians have no memories, they have completely forgotten, a snake is a snake
zonsezi ndi a Mbendera galu wa chabechabe.cheque book judgment muphesa mtundu wa amalawi.
I agree with you comment for 72. I was shocked to learn Malawians had brought back DDP. I just wondered if they were normal people. Now they can see for themselves, what they created. They are people who never learn. What a pity. Which donor can give DDP money after all DDP did. They are not stupid. It is their tax payers money who work hard to earn that money.
U r stupd e 1 edtad dc post had t bn i knew t b4 i cud let e nonse c mata 2 go ku nkhongo,ukhale dona iweyo ngat sungataye mtiwa,bwanj sudaimire kt u cud comvinc thoz so called donaz? UMBULI BASI KAGWERE MULEKEN P.A.P.M قیحفقب جنشطبچسب!
I was totally baffled in May when I saw that Malawians had elected the leader of the DPP. Malawians must have very short memories since they seem to have forgotten all about the chaos left behind by Bingu of the DPP just a few months earlier. Can a leopard change its spots? APM is the brother of Bingu. Why should he be any different? It is not easy to find a way to hold another election when the MPs of the DPP would never pass a vote of no confidence in their leader. It is futile complaining about the President… Read more »