Email a copy of 'Mutharika visits floods victims in eastern Malawi: Pictorial' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

63 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Rodrick Mbuya
Rodrick Mbuya
9 years ago

kikikikikikikikikiki ndipo anthu omwe nyumba zawo zili mmadzi sanawafikile anabwelera pa main venue ya function yakeyo. Anthu ten ndikulandira ma blanket ndi nyemba 10 kgs chimanga chinabwelera osachigawa

Eliam
9 years ago
Reply to  Rodrick Mbuya

Nanunso inu a Rock President sangakwanise kuyendera anthu ovutika ndi madziwo khomo ndi khomo. He is very busy man @this time. Pls write sensible mufwetu.

Malawian
Malawian
9 years ago

Some people just like to criticize basi. What matters is that the president went to visit the affected areas n saw mavuto omwe anthu akumana nawo. Zoti anavala suit zilibe ntchito. Thats nothing. Its not even an issue. Why anthu enanu mumangopanga criticize zinthu mwa emotional n personal?? I mean even osachita manyazi kupanga post such type of comments? Come on lets be objective n sober in our criticisms. Seriously nkhani yazovala seriously??

Mwanapwa
9 years ago

Limeneli likuoneka kuti ndi bulangati la anthu avutikitsitsa osati omwe akupelekawo. Zikomo bwana president

Phillip
Phillip
9 years ago

I have been reading some comments which suggest that the president was ill advised by wearing a suit at his visit to the disaster area. Well in my opinion i don’t think because wat he was wearing was not a suit at all. A suit is a jacket and a pair of trouser that looks a like. What matters most is the intention and not what wears and after all for earth sake it wasn’t a suit. The only error they did was to put the red carpet.

ben kamwendo
ben kamwendo
9 years ago

im very thankful the pipo who trying to help malawi God bless you

ben kamwendo
ben kamwendo
9 years ago

im very sorry for all malawians although am in south africa. I will also try to help some of them its very sad story but God is with us

dyton Chiwaya
dyton Chiwaya
9 years ago

Iweyo ukunyoza ? Iweyo wapereka chiyani. Khaya bulangete ndi laling’ono pena ai none of ur concern. Bravo Peter. You are moving in the right direction

Angaliba Nusufi
Angaliba Nusufi
9 years ago

Enawatu akufuna alemererepo ndithu. Chithandidzo bwana wathu ndiye wapempha ndipo chayamba kale kufika mdziko muno. Tingowapemphanso abwana omwewo kuti apange zothekera kuti anthu okhawo omwe ali oyenera kulandira thandizoli alandiredi. Chifukwa monga tikudziwa tonse kuti “UMBANDA” wakula kwambiri ku Nyasalande, let’s just pray kuti ntchitoyi iyende bwino ndi kukafikira awo amene ali okhudzidwa.

denis tembo
denis tembo
9 years ago

Nkhani yomvetsa chosoni,

Chris
Chris
9 years ago

Can someone please tell me how to go about to donate some money. I have about K200,000 that I feel can go long way my problem is am in SA. Please can someone or an organization send me an email on [email protected]. I really feel for the affected people and I Pray to God to give them strength.

Read previous post:
Action/2015 Malawi calls on govt to localize international development goals

Action/2015 Malawi has called on government to localize international development goals for positive results on the ground. The group is part...

Close