Email a copy of 'Mwawi’s call up snub angers Netball Association of Malawi' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Mwawi’s call up snub angers Netball Association of Malawi' to a friend
A Lilongwe couple is admitted to Kamuzu Central Hospital (KCH) after the man allegedly chopped off his wife’s hand following...
Kodi mukunena alomwe? Aaa! nivindere ivi. Njelu vilijeso, kweni unkhungu pera.
Bati mbweno bakkulira bati. Kulira Mwawi. No soni! Wanozga iwe wa mwana Mwawi iwe!!
Kirininti, whatever u call urself, ma northerner, akulakwira chani, after all netball team yo ambiri ndi akumpoto, flames ambiri ndi akumpoto. Phunzirani kukonza pomwe palakwika osati chamba ukusutacho, pathako pako. Anthu akumpoto tinakulakwirani chani? Mumazimva chan inu? Nzeru simutiposa, mumatiposa kuchindana kokha, nchifukwa mumabeleka ngat chiswe. Tikukulemban ntchito ku ma estate afodya . Zopusa!!!
Mu haahaha kkkkkkk koma Mbuzi iwe e. Asikana amulakho amaziwa kudikhula Selebwede dance basitu…
mwana akayamba kunyoza kholo, ndiye kuti wayamba zibwezi. akatenga mabomu ndizina kumeneko, azalifuna kholo. Today has money to get a dentist in RSA, tomorrow she will need gvnt support. she knew the games earlier, why didnt she communicate to NAM before the call up? Akumati akaona mmusimu akuzimva kukula.
The young woman holds a high position in the Nyika Secession Movement and she thinks she is fighting the current administration by snubbing NAM’s call up. Please let her go, mtumbuka wachabechabe uyu. Replace her with a Malawian not another Northerner.
Mtumbuka nayeso wakwiya sakufunaso kumenya mpira mu team ya Malawi. Akufuna federalism itheke kaye because tsankho alomwe inu mwawonjeza. Alomwe ntchito mkupanga chigololo ndi kusankhana mitundu basi, kumenya netball simutha mumangopwisa basi after kukhuta nandolo. Vi angulu vi wanthu vokonda kudya njoka. Bravo Mwawi mwana wa kwithu kukaya!
No. 1 ndiwe munthu wanzeru ndithu. Kodi mukwiyowo ndi chifukwa cha chiyani kodi? Nsanje ndi Mwayi, Kuonetsa khanza kwa mwayi or puti ndichiyani. Iyayi, kafuneni kwa goliati, Chimaliro, Chonde basin mupeze wokondedwa wanu azishaina.
She is there because of Malawi govt and Malawi netball? ????? NO NO NO THATS INCORRECT. Ali there because of Luso lake/ talent that God gave her. If people play professional soccer or netball because of Malawi government then you should be sending thousands out since you have the capacity kkkkkk
mwasowa zonena munthu asadwale? Go you will lose miserably. …
I see we hv a problem here. Mwawi and NAM hv issues to sort out as it is an inside issue and to the Nyasatimes reporters plz b4 u publish any article it’s better u verify the source of an issue and pipo involved, when evidence is tangible then u publish. As 4 now names of pipo wil be pulled in the mud. Sumthing is cooking sumwhere. Resolve the issues now b4 the can of worms are opened.