Malawian arrested in UK for shoplifting

Khan: Arrested
A Malawian national living in Bolton, England is under British Police custody after being arrested following a shoplifting incident at a clothing store of TK Max.
British Police arrested Andrew Khan was allegedly caught for shoplifting female clothes.
Khan was arrested on a misdemeanor charge of shoplifting. His girl friend [name withheld] has been informed,” said a source.
Pals of Khan told Nyasa Times that he has been under arrest on suspicion of theft after he allegedly failed to pay for bras and gym wear pants.
He is said to have been getting the pants for a Malawian girl friend who is in the British Army who had asked for them.
Tagged with: Andrew Khan, TK Max








Pamenepa ndiye timati recession yafikapo.Nawonso asikana achinyasa anyanyila ma demands kwambiri.ma shift atelela koma chi lisiti chofuna zithu thothotho…akanapanga bwanji munthu kuti apatu ndikapusa game ija sindiionanso.nkhani zake ndizimenezo.Koma mwamuukira nkhani ngati ndiye inu anthu olongosoka.Nkhani ya Khan yatikwana kwabasi…koma makaladi eni eni mmene ndiwadziwira ine amakonda kuba ma engine amagalimoto akutha pa Malawi ndikuwunjikana limodzi panja pa chocolate city mazulo ka elephant kotentha manja ngati anthu ozindikira kwabasi…kuno ku ulaya mwenye ndi nkaladi sayiwothera kwa mzungu.Tiana tabwino tachizungu timakonda akada ife kwambiri..ena ndikumataya nthawi kulimbana asikana apa nyasaland akuvitisani ndimiwado ya TESCO VALUE.
its okay