Email a copy of 'Njobvuyalema attacks 'clueless' Mutharika over Malawi economic revival' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Njobvuyalema attacks 'clueless' Mutharika over Malawi economic revival' to a friend
Ministry of Agriculture officials have issued a temporary ban on livestock slaughters, insurance of livestock permits and suspended all livestock...
Kkkkkkkk,kunyasisa nkhope bwanji iwe njovu,nkhani ulinayo ndiyoti umafuna udindo osati iwe mkusintha zinthu.Njovu ta chabechabe.
Kkkkkk koma kumalawi…… Aliyense ali ndi mzelu zoyendetsera dziko kkkk koma a nyasa mumusinthe munthuyu picture yakeyi,,, sibwino choncho…
tazingolimbikirani kugwira ntchito basi. Zala lende mwati bma lizingokupatsani za ulere? Simukuona anzanu tikudzutsa ma mansion mmataunimu inu mubalirabe choncho. Dolo ndi Jessie, wati ziiii, waionera patali.
Koma DPP ndi mbola amwene.
Peter should be booted out.
It time Pitala stopped saving the asses of his cashgate friends and himself so that the aid taps started flowing again.Nothing is working with his useless zero aid budget.Its time he worked on 577 billion cashgate than relying on some non working zero aid budget.The way the kwacha is falling,we are soon going to reach Zimbabwe levels.This useless professor should simply admit that he has failed Malawians.Malawians are finding it tough on everyday basis.
DPP ndi mbola amene akubakila apm ndi alomwe! Ndipo amapeza zinazake.things are getting worse everyday tifika PA Zimbabwe. Athu okuda simungayendese ziko mukuchepa zofunika azungu akhalepo. Mwaiona Zambia???? Mayi Joyce banda bweran muzatiombole Ku 92 billion hahahahahahahah a DPP osalusa macheza awa
Its easy to spot out mistakes when u r out of field of play
Capital Radio please repeat this interview. you are the best râdio.
Indeed Malawi cannot survive without donors. It’s not about DPP it’s about the freezing of aid but now Mutharika & his friends need to do the right thing to win back the donors.