Email a copy of 'No apologies, MCP tells Mutharika: Malawi News hits at ‘senseless’ opulence' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

120 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Innocent Blacknyasa Pembah
Innocent Blacknyasa Pembah
8 years ago

Malawi is in pain.. Mwatikwezera passport kuti tifere momwemuno. Tikayamba business mukubadwitsa timisonkho topanda mitu, school ndi iyi mwachotsa PSLCE ndi JCE yet MSCE ndiyomwe yaphweka kubeledwayi… Bursery mukuti yathanso amphawife mukutiganizira? A super rich african american who made millions of dollars in america, why is he here in malawi the poorest country on earth? Ngati muli ndi ndalama mudadzikwezera salary yanu chifukwa chani? Misonkho ndi iyi mukutipha nayoyi, mukapanga zopusa anthu nkudzudzula muzitiopseza pomenya matebulo? Musaiwale Lucious Banda adaimba kuti boma salamulira pomenya matebula koma mofatsa ndi mozichepetsa… A super rich president athu….. Musaiwale kuti amalawi akatopa amanena momveka… Read more »

Nyakulama
Nyakulama
8 years ago

ministering to the pple is different from ministering to God. 2019 DPP will continue.2024 to 2034 DPP with Dr Chilima.Politics is a game of numbers sizapagome izi.ngati mukufuna kulamulira mpofunika mupange convice southern region & the entire Lomwe.ForYour Info. registered Lomwes who attend the muhlako wa a Lhomwe is over 5,000,000 pple across the nation. ndiye pali ena not registered, mukhaula simudzalamulirapo. zizingokufinyani mumtima.dziko ndi lathu ili, we are everywhere in mw in large numbers.

George
George
8 years ago

Manowo timaliza ife za utsiru sitimafuna Gyz tiyeni tiyende pa 20 pakubwerapa

marvel chikondi
marvel chikondi
8 years ago

MCP still habours the dream that it won the general elections. again you can see that their leader after leaving God has lost directions. he thinks only of power & ruling Malawi. as a veteran in the field of scripture he should have advised his followers that everything has its time. DON’T RUSH

weniweni
weniweni
8 years ago

Akatolika munyengo ino ya kolona tiyeni tikumbukile kupemphelera dziko lathu,ndithuuu.otherwise eiiiish, we are heading for crush landing ndukuuzani.

Mlomwe
Mlomwe
8 years ago

Wamva Peter?ndi mutu wako wowumawo

Mlomwe
Mlomwe
8 years ago

YANKHULA MAYI WANGA.KODI A DPP KALIATI WANU UJA ALI KUTI?KODI DZINA LOTI PATRICIA KALIATI LIKUPEZEKERA UNIVERSITY YAKE ITI MU MALAWI?FUNDO NDI NZERU ZILI MU MCP.UKU NDIYE TIMATI KUYANKHULA MWACHI MALAWI

Austin Banda
Austin Banda
8 years ago

If you had posted the word of God so many people could have been inspired and saved in this last hour of our salvation.Lets fear God and give Him glory for He made us in His own likeness.Lets love one another for we are the temples of God in whom He dwells.

maliwa wa chamba
maliwa wa chamba
8 years ago

The significance of the truth is that it pains and nothing shall come to pass before it i s revealed. Midnight boma can not produce tangible things because it is passing with the angel of darkness and death. Bravo Kabwila. Very soon God is going to reveal Himself of the truth of the matter.

Mtondoli Jonazi
8 years ago

I think nthawi yakwana yoti ndidzakhale president pa Malawi. The following is the list of my do’s and don’ts: 1. I will not stay at the State House. The government will just have to do with nyumba ya housing or yotchipirapo mu Ndirande, ku 18 ku Lilongwe ndi ku Masasa mu Mzuzu. Better still ku Mzuzu I will operate from kumudzi ku Jombo, Enukweni, Mzimba. 2. Draw a MK1.00 salary because I will need to get paid as per requirement being a government employee 3. I will not need a body-guard? For what? Kuopa kuphedwa? I doubt if I have… Read more »

Read previous post:
Lucius Banda says all set for Malawi Sand Festival: Busy Signal confirms performance

Jamaican highly rated dancehall artist, Busy Signal has finally confirmed he will perform at this year's Sand Music Festival after...

Close