Email a copy of 'Nsanje registers 3000 primary school dropouts' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

11 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
DaDa
9 years ago

Federal system ikuchedwa tisamamve nawo nkhani zopusazi.mwana kuthawa ku xul ndekuti chani???

Richard Pankomera
Richard Pankomera
9 years ago

This is literally bad!! we need to introduce compulsory free primary education NOW and not later!!

....
....
9 years ago

Ali mtawuni muno ati “thandizeni bwana”.

bwampini
9 years ago

Nanunso a Nyasa mudziona nkhani zolemba ku nsanje kungakhale ophunzila… Bola kumpoto kkkkkk

kwa phelewera kwathu
kwa phelewera kwathu
9 years ago

Nawo alomwe ndi aSena ntchito kukoka makutu basi.school ndi imeneyo mukuyithawayo.koma mmawa lino mufuna kuti mukhale ma president muzizazunza anthu basi. Zonvetsa chisoni.mchifukwa chake boma langoganiza kuti likubeleni ndalama muonjezere kokagulira zida zo kokera makutu.

mabilinganya
9 years ago

This is a shit of a country!!! Forget about development

duduzi
9 years ago

Mwayamba kuyithawa nokhatu……..timakuwuzani kuti sukulu sachita kukakamiza ayi …KUYESERA KOTA koma AYI ndithu…..koma kulimbana ndi Mtumbuka ndi Northern Region yonse. Zitsiru kwambiri …..inu makamaka former Vice Chancellor wa UNIMA, Chapola ndi Bingu(do not rest in peace but burn to the bone in a hell of fire …for causing all the sufferings of the Northerners). Izitu zili ndi anthu kapena mtundu wake wa anthu olo chigawo………mwana Mpoto amakumana ndimakondishoni oposera pamenepa koma osayitaya sukulu ayi ndiponso no marriage arrangements kumene kuja. Nchifukwa chake mumaberekana ngati ngumbi – a BLM, PSI kuyesetsa kukuphunzitsani kulera koma ayi ndithu…..mapill olelera kukataya komanso nyama kunyama… Read more »

A chimwene mwalalata
A chimwene mwalalata
9 years ago
Reply to  duduzi

Akulu mwalalata inu. As a southern man, I am disappointed with these girls and especially their parents. I have been to the north, the motivation and material support that parents in the north give to their children is enviable. Too much poverty in Nsanje, occupied with what to feed their families tomorrow, what else could the parents of these children do? I am upset with our politicians, dam shire and any other river in Nsanje, get massive rice farming schemes going and start making a difference to these peoples lives. A sad lot of politicians we have: a sad lot… Read more »

womenslib
womenslib
9 years ago
Reply to  duduzi

You are a stupid and divisive fool. People in Nsanje have always been kept poor. These are the consequences of years and years of being ignored by the ruling governments and being treated as if they were foreigners in their own country. It’s idiots like you that will cause civil war in the country with your inhumane racist…yes racist and insensitive comments. If Malawi were to become federal your region will immediately be destroyed if it’s being run by idiots like you. We are a global village now. If you don’t understand what I’m saying by a global village take… Read more »

faines
faines
9 years ago

Zonsezi ndi a Tumbuka ozikonda. Kufuna kupanga distract from yopanda zimbudzi ija. Mwang’omboka

Nyaka
Nyaka
9 years ago

Choncho nanga mkutani? Kukupatsani Kota ayi ndithu. Sukulu mukuyithawabe.. Anthu osathandizika Inu. Mukatha Apo kutukwana atumbuka.. Mxi!

Read previous post:
Advantages of federal system of governance in Malawi

Localized Governance Every province has political, social and economic problems peculiar to the region itself. Provincial government representatives live in...

Close