Email a copy of 'Of nurturing criminals: ‘11 Bongos’ gang in Malawi' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Of nurturing criminals: ‘11 Bongos’ gang in Malawi' to a friend
A 28-year-old man is in Police custody at Balaka Police Station in eastern Malawi for allegedly impersonating a police officer....
Just shoot them
Sizowona akuyenela kulandila chilango chokhwima
11 bongos izabwere kunyumba kwanga. muzangomva zothaitha nditaphulitsa mitu ingapo ya akapolo amenewa ndi onga wazipolopolo. Ukawauza apolisi akachasowa palibe amapanga. Kkkk nanga apolisi nkumati tili nawo kumanena achina Kaching’ona akukawale? kkkkkk kachaso ali mbweeeeee mthupi.
Ofunika kumanga kaye mafumuwo coz ndi ana a azibale awo.akaulula.
Zonyansa kwambiri!!!!!
Let Military Police go to that place and clean it of these notorious beasts. Our police is a disgrace, how can they fail to deal with all the gang members?
We are scared of these dreadful creatures.Even the feared Ndirande inkatha cannot do anything to these weed smoking thugs.There role models are boko haram thugs.We are locking ourselves in houses to keep away from these blood baying thugs.They have totally gone mad at the moment.Even some girls joined them like the Pinks girls.These girls can fight like men.
Where is the army? kwathu kuno kulibe nkhondo, ngati apolisi achepera the army should come in to wipe out these headless mbuliz.
ABWERE KU NDIRANDE KUNO AZIZABVUTITSA….TIDZAWAPHUNZITSE ADZAONE CHIDAMETA NKHANGA MPALA… PLEASE….KUNO MABONGOWO TIMAGWIRA KUMENYA NKUPHWANYA NDI MIYALA KUTSILA MAFUTA NKUOTCHA…..SITIMANYENGELERA… A POLICE AMAMANVA ZOKUTHA…..!!!! KU AREA 36 KU LILONGWEKO CHANGAMUKANI… UMBUZANI IPHANI APOLICE AZINVA ZOKUTHA ITHA…..CHIFUKWA PENA AMAHONGEDWA NDALAMA…..NDI TIMIGODI TAWO….
Where are our poloce officers