Email a copy of 'Off the wall of Dickson Kashoti: Mutharika joins the foul-mouthing politics' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Off the wall of Dickson Kashoti: Mutharika joins the foul-mouthing politics' to a friend
Ugandan comedy queen Annie Kansiime will tour Malawi again in July as she is expected to perform at Bingu International...
Bwana tiuzeni yemwe anapha Robert Chasowa ku Poly, yemwe anapha anthu 20 in July 2011, yemwe anapha Issa Njaunju. Kodi onsewa anaphedwa ndi MCP? Mumafuna kuti anthu akutameni ngati mumatha kulankhula bwanji??? Anzanu akyamba kubweza moto musandaule kuti akukunyozani. Ife timaona ngati mwapita kumpoto kukapanga msonkhano wachitukuko, koma ayi mumakapanga msonkhano onyoza anzanu. Za ziiiii.
Man Mutharika tiye nawo akanganyawa asakuzolowere. Anaonjeza mwano koma tsono uwauze chomwe iwo ali, makamaka this toddler in politics one Laza Judas the Iscariot uyu adachita kuthawa pa pulpit nkumaganiza kuti azitiomba akamabera dziko lonse mmene amatibera ku Assemblies.
“Mutharika joins the foul-mouthing politics”? Bwana Kashoti you have rightly put it. This statement “Mutharika joins the foul-mouthing politics” means that Mutharika never did foul-mouthing politics while everyone else was. But through observation learning, you have taught him. Who is to blame now?