Email a copy of 'Parliament staff goes on strike: Malawi MPs meeting for mid-year budget review' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

24 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Mu umodzi muli mphavu
Mu umodzi muli mphavu
9 years ago

Zopusa basi, achotseni, ntchito mulembe ena .kwachuluka mahule kumeneko.

mmalawi weniweni
mmalawi weniweni
9 years ago

Zopusa! Idislike stupid DDP. Inu poyipatsa mpando DDP yanu m’maganiza zizasintha? Fisi ndi fisi basi angamile m’madzi sadzasintha kukhala ng’ona.

Zachisoni Phiri
Zachisoni Phiri
9 years ago

Za ziii

pina
pina
9 years ago

Akupanga strike panopa popeza mwalowa ndalama za donation for floods akufuna adye ndiwo osati anthu akuzutikawo. Yet mukugona pouma, tea daily wamkaka, myama daily pa table, osanganiza za anthu akufa ndi madzi wo…

Malapwalapwa
Malapwalapwa
9 years ago

Tangolembani ena basi,malovatu ife tilipotu ambiri kwabasi.

Hannockie kambirinya
9 years ago

zopusa basi

Amachita strike akulira maliro afloolds mulibe manyazi ndi chisoni eti ? Konyani

Amachita strike anzanu akulira maliro a ma floolds mulibe manyazi osadikira kaye tilire kaye bwanji?

Ramsey Majiga
Ramsey Majiga
9 years ago

Ingowachotsani ntchito basi ” Just fire them all” nothing else.

Wachangu
Wachangu
9 years ago

Zamkutu

kadyakolo
kadyakolo
9 years ago

apatseni antchitowo maright awo kodi zimakoma kubera mavoti basi uchenjere mpando wakowo upita kwa tupele unangothandizira kubera mavoti ndinena iweyo chilima galu wachabe chabe

Read previous post:
Shanil warns against abuse of relief items

Former Malawi First Lady Patricia Shanil Dzimbiri has appealed to authorities tasked to distribute relief items to flood victims to...

Close