Email a copy of 'Police Commissioner Matinga dies after collapsing during meeting' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Police Commissioner Matinga dies after collapsing during meeting' to a friend
Opposition leader Lazarus Chakwera has called the Democratic Progressive Party (DPP) led administration as “inconsistent government” and that the nation...
aah anthu abwino sakhalitsa.can we learn from them ossti ubissla kyseli kwa mtengo ndi ma camera sti kugwura a iver soeed pamene iwo akufuna over pocketing ndipo camera calubrsted below legal road limits why amakawi why .actually ku rsa konko you seen how vehucles move ma freway joxi vua bitbrudge to mlw or jozi via nedprit to maputo….. mwawonjeza unu aku ares30 ma receipt malemba aja si a fake nbrs overprinted and why tikspita kwa cashier no recordd licence matengelanji ngati pachitika nhoxu nsnga insurabce vovets whst!?
zopsezanazu ayi?
Rip
very humble senior police officer. Tasewela limodzi pool pa Jacaranda bar ku Mzuzu. Kucheza nawo munthu sungadziwe kuti ndi bwana koma tima inspector sikudzitukumula kwakeko. RIP Matinga
Mwalirika bwana ndi mtima wanu wabwino. Yonse a Malawi ifa yanu yatilitsa. Tisowa anthu anzaru ngati inu mudziko lathu lino. Chitsanzo chabwino mpolisi munthu wophunzira wolandira ndarama zambiri koma Ana awiti okha basi koma olandira ndalama zochepa Ana 8 Chaka ndi Chaka. RIP bwana.
Zovuta kwambiri. May his soul rest in internal piece.
RIP mr Matinga
Mayooo! Ineeeee.
MHSRIEP.
RIP Mr matinga
Kumanda kunka anthu anthu, kungosiya zitserekwete za cashgate. I will always remember you ( Mr Matinga) the day I came to your office in Zomba last week when you came down the stairs escorting me up to my car despite your being superior than me in everything. You were my role model in both your profession and manners. I will always remember you!!
May your soul rest in ertenal peace!!!!!
Abwino anzeru kumapita usiya a cashgate mmmmm mzim wawo uuse mu mtendere. Mulungu wskukondetsetsani zedi. Tilinanu pamodzi achibanja pa chosni chimenechi