Email a copy of 'Police erred on MCP arrests – Malawi Law Society' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Police erred on MCP arrests – Malawi Law Society' to a friend
Malawi government has said it is taking “seriously” allegations that there has been a plot to overthrow government and police...
Very sad indeed, it’s long way to go before Malawi will get out of poverty. Our leaders are busy fighting each other yet us the voiceless are suffering. no jobs, no development, no food, no clothes, no money no drugs at our hospitals. This is bad, very bad indeed.
Govt now has egg over its face. These people must be compensated. Heads should roll. We don`t want to go back to the dark days of detention wityhouttrial
kodi odandaula omamunjataso?yee!!wanthu oludandaula kuti zinthu sizuyenda bwino,ndiye mkadatinjata poti tsano tiyamba kulila zamalipilo ya wanthu ogwira ntchito ku boma,ayika otsibweni msatinjate
Thumbs up Kabwila. Keep on fighting for us. Achoke!!!! achoke!!!! achoke!!!!, achoke anyaphaphi amenewa. anabera zisankho, alowetsa chuma pansi, akulephera kuthetsa njala, magetsi adakazimazimabe. Ndalama zikusowa, anthu akulephera kupeza 1000 kwacha ya mgaiwa. Katundu akukwera mtengo daily. Akulephera kupititsa Bill ya ATI ku Parliament, akulephera kukopa ma donners kuti ayambe kuthandiza dziko lino. Ndiye chimene akukhalira m’bomamo ndichani.
kabwira keep up fighting for the rights of the voiceless. this is the party that I know which smoke out those who advocate the public concerns.I wonder why the police dance into the tune of the party rather than protecting the citizen at large. Am afraid to warn APM that what the police is doing is mismanagement of public money bcoz lawyers to deal with the issue at hard will be paid instead that the money would have been used to construct a block at Katunguwiri which has been a junior secondary for aperiod of a decade and half. My… Read more »
Akudikira kuti Parliament ithe. Muona adzaziyambaso nkhani zimenezi zomanga anthuzi. Pali ndae yauchitsiru apa
Jessie, that is the politics you preferred to join in 2013 when Bingu was alive. Politics and arrests are twin brothers. Ask Kizza of Uganda, that’s African politics, this keeps those in authorities alive. Read more about politics. DPP simumaidziwa mayi apapa ndiye muidziwa nthawi ija munali outside politics mumangopanga noise ndiye analibe nanu ntchito apa muli mkati mwa politics mudziona amama Kabwila. “Politicians are not the people to be feared” 2009 Dr Jessie Kabwila Kapasula.
Zachisoni pa nyasaland
Zili kumalawi kkkk
VERY SOON YOU WILL SEE THE KWACHA STARTING TO REBOUND. CHOLINGA AWABERE ALIMI PONAMIZIRA KUTI KWACHA YAKWERA MPHAMVU. THIS GOVERNMENT IS CROOKED!!!!