Email a copy of 'Police impound surgical medical drugs, Cannabis' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Police impound surgical medical drugs, Cannabis' to a friend
Malawi Hip Hop artist, Gwamba, will have his first appearance on international stage as he is billed to perform at...
Divala marry me pliz, you are beautiful to be a police woman, I willl send you to school to be an accountant. You are very beautiful woman
Being a police officer doesn’t mean 1 is uneducated. FOH
Nzeru Ana a zaka zochepa akatenga kuti ngati okalamba akupanga zoipa ndi Ana omwewo. Today u find a 55 yr old undressing and showing his nakedness to young. girls ulemu wapita kuti. Umunthu wathawa kodi? Tikulowera kuti. Zamanyazi ndithu.
koma yea MTL yatchuka pitilizani uchifwamba guyz!
POLICE NOW YOU ARE COMING !!!!!! KOMA CHONDE CHAMBA ICHO OSASUTA.
A 70 years old man and a 30 years old woman in business? is this parasitic partnership or marriage?one will remain a looser
MTL is full of criminals. Some of their own have settled in Ntcheu and Balaka and continue with criminality. Shame!!!!!
Legalise marijuana, bola kugulitsa chamba kusiyana ndi uchifwamba. Let them go coz akuthandiza kubweletsa forex.Comment
Koma azimayi ambiri ayamba kutakata ya mankhwala ozunguza Bongo masikuano bwanji? Kodi profit ya uhule ikumachepa eti? Madolo mukumanenelera kwambiri mpaka ena mukumadya ngini ya ngongole
Chamba chimalimidwa, kutengulira, fertilizer application, kuthenela, kuchikhwimitsa, Harvesting and selling to Dealers, apolice konse kumachitikila izi amadziwako amafuna akakumangani chomcho katunduyu akagulitse ndi iwowo, Divala chamba mwagwila nthawi yaitali panopa matumba osawelengeka, ndilitilo munauzapo amalawi kuti chamba chija lero tikukaotcha??? Mukuyang’anila muvi bwanji osamanga ma Growers achambawa ndikuotcha mindayo U will see owoda chambawo asowa kokachipenza koma Ridiculous basi!!!! Apatseni chamba chawo amachapila Tsitsi!!!
anjatidwe ndithu amenewo. muzipatala mukusowa mchape iwo ndiye azingoba?