Email a copy of 'PP admits elections loss costly: Matola tells Joy Radio party rebuilding' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'PP admits elections loss costly: Matola tells Joy Radio party rebuilding' to a friend
A businessman thought to have run away from South Africa for criminal offences has been traced to be in Malawi...
Nawe anthu angataye nthawi kumakomenta za pp lero. Musiileni msonda azikomenta.
BAMBO MATOLA CHIPANI CHINAGWA CHIFUKWA CHOTENGA NYANSI KUYENDA NAZO PAMODZI. MASIKU ANO ANTHU ACHANGAMUKA. INU MUNGAMAIKE PANTSOGOLO AGATAMBWE NGATI LEMANI; ULADI MUSSA; ZIKHALE NG’OMA TAONANI PANO KULI CHUUU….IDANYAMUKADI ILI KUNJA…..AMAYI NDIYE ANAWAZA SABWERANSO AKUOPA CHAKUDA
Chipan sichitha,musathe mau ndi ma comment opusawo,itini phe muone
Pp idatha and sizabwelanso ayi
Remain strong PP, the only party which tried to embrace the whole country. Let political prostitutes leave, 2019 join forces with MCP and help develop the whole country Malawi.
A Matola mukuti bwanji? Kodi PP iripobe ifetu tinakwiriratu chipani chimenechi.kkkkkkk inu anthu a PP musandiseketse inu nkutenga anthu monga BJ Mpinganjira, Uladi Mussa nkumati muwina masankho? Inu mukuoneka ngati nzeru zolamulira dziko munalibe pamodzi ndi mayi athu aja. A Malawi sitinakufuneni and no matter what PP could have not won that election. Mukamfunse m’bale wanu Gwengwe inu a Matola. Gwengwe kumuuza za PP akhoza kukupatsa mbama coz this PP wasted his time and resources. PP won’t rule Malawi again mark my words.
Adanya kutenga nkhalamba mchipani mwaomodi
People thought DPP will never rule until the time they were reminded kuti Amalawi sachedwa kuiwala. Ingotini pheee
Pp siiwina but pitara. Eh headless
Munakanika kuwina muli pampando ma resources onse aboma (at your disposa)l ndiye pano mungawine? Chipani cholamura chantundu wanji kukani kuphika ma Plan obera? Ha ha ha ha ha ha ha nzimayi ndi nzimayi basi!
WITH DOUBTS FOR PP TO WIN 2019 ELECTIONS, SORRY TO MENTION THIS BUT STILL NO HOPE OK.