Email a copy of 'PP's Msonda describes Maulidi as confused, desperate man' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'PP's Msonda describes Maulidi as confused, desperate man' to a friend
The future of the railway project under the Brazilian firm, Vale Logistics Limited faces uncertainties as some Malawians in other...
DPP ikundimvetsa kukoma ine
inu a sibweni wasowa zokamba mwangodana naye musondayo. musonda ndi mneneri wa chipani chathu cha pp amanena zimene chipani chamutuma.
Ife a pp amene timakhla naye kucheza naye kudya naye tsiku ndi tsiku tikumuziwa musonda makhalidwe ake tifunseni tikuuzani. amacheza ndi aliyense wamkulu mwana abambo amai wolemera wosauka angakhale amasikini amamukonda. musonda ndi atsogo athu timamunyadila kambani zina za chigololo mwanama. more fire musonda maulidi sayamika wadya zambiri za amai pano wayamba misala kuluma chala chimene chikumudyetsa satana jabulosi
Its Msonda who is disgruntled,desperate,confused & frustrated.Munthu wa nzeru sangamasokoneze banja la mzimai wa mvano ku Chilomoni.mamuna kupanga busines ku Mangochi sindiye kuti mkaziyo ndi wanu.Asiyeni aMaulidi akupanga zandale inu siyani chigololo basi.
CHIPASUPASU CHA ANGONI PAMATENGO/ELIKO WAZUNGULILIDWA/BABULO AKUGWA.
ANSONDA MUWASIYE A MAULIDIO TIWAGWESE.KUNO KULI PHISO WA DPP. IWOWATU ANAGWAPO KALE KUNO KU BT NORTH NDIPO SANATUKULEKO AI.MUKUWACHOSA KUTI MUSALE A YES BWANA OKHAOKHA BASI.AGALU AMISECHE INU.
Musiyeni mzanu, awina basi. Ife tivotera ameneyu kwathu kuno ndiye musamuletse.
musiyeni Maulidi Pauloyo ayime awone yekha.kuti tsopano kwake kunatha. bambo Maulidi mudzakomoka ndizotsatila ingosiyani, nthawi yanu inapita ano ndi masiku a anyamaya.
Kodi uyu waufa m’mutuyi amadya koma??? Musiyeni Maulidi azionere yekha paja DPP imawawitsatu ndipo Joyce akudziwa bwino nchifukwa chake anaiwala mwado yake ku Sanjika.
JB analumidwa ndi chakuda ndiye sakufuna atamvanso liwu loti election