Email a copy of 'Rev Maulana re-elected CCAP Blantyre Synod SG: Chimkwezule is spiritual father' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

37 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
GADABWALI
GADABWALI
8 years ago

Mukunyadzitsa dzina la Mulingu azibusa adyera inu. Kufuna muzinyabita chopereka basi? Kulimbirana maudindo, wat for? Mukatha Apo mudzikagona ndi ana and ndi ma house girl nkumawapatsa pha. Wat msg are u preaching? Kukutchulani Zidzete si kulakwa abakha inu. Were u really called to serve God? Ndakaika.

Cash Gate
Cash Gate
8 years ago

congratulations

gojo
8 years ago

koma masiku omaliza kkkkkk

mwalawira
mwalawira
8 years ago

No. 25 Please, apologize and ask God to forgive you. The people you are cursing are pple who are anointed by God. When they make mistakes it is not for you to judge and condemn. Let the appointing authority ,God, do it. Don’t invite tsoka on yourself.

Harris Bonongwe
Harris Bonongwe
8 years ago

It is very unfortunate that the elections went ahead despite of all these wrangles. to say the truth we have seen the work of the devil at its best. nkhani za church kuipa kuposa za ndale. who doesn’t know the evil that men like Maulana, Jumbe, Mbedza, Chikopa Innocent and the rest of them does? All these men wants its security and riches and an easy ride though they are the worst we have ever seen!! Mr Jumbe mowa uja anasiya otochita kukhala nawo pa counter?? Innocent Chikopa hule la munthu, and using St Columba church to enrich himself!! pano… Read more »

Mwisho
8 years ago

Khalidwe la Ncozana taliwona bwino tsopano. Sakusiyana zochita ndi ana a pa Poly. Staging a strike before thinking and yet imvi zili thooo m’mutu. Phuuma too much a ncozana. Why walk out of a conference when he was supposed to be part of the solution? U doctor ndiye uli pati apa?

mercy
mercy
8 years ago

Christians, you need to know that these are signs of the times, the anti-Christ are taking their stand against the true worshippers. But we have the living God who knows everything because He is Omniscient, omnipotent and omnipresent and He, God will show us the truth at the end of it all. We just have to be patient.

Kachingweh
Kachingweh
8 years ago

Tiyeni tilimbikile kupemphela bola tikapulumuke chipulumutso aliyense ndiyekha not synod.

mulibwanji?
mulibwanji?
8 years ago

Ncozana & Kadawati zitsiru za anthu. Mesa mumaziti abusa osonkhanitsa nkhosa zikasochera? Bwanji apa mukuzibalalitsa? “Akuwoneka a Uzimu koma mphamvu yake anayikana kale….” Azibambo adyera.

Ndiye mwapusatu….kunalibe ziwawa mumafunazo. Azibusa anji osogoza satana mmalo mwa Mzimu Oyera? Chitani manyazi akamberembere inu. Imvi tho! Ngati zenizezi. ZITSIRU!

Kadawati
Kadawati
8 years ago

Ncozana is from central region Lilongwe to be specific. Why is he allowed to confuse our beloved synod? Rev Maulana is the best GS so far amapanga zake salimbana ndi munthu. Chimesya akungoyenela kusova basi. Eti kumachita kuzitamilila kuti ndi wa PP? Let God’s will be respected in the synod.

Read previous post:
‘Judge shopping’ warning from Malawi Chief Justice

Chief Justice Andrew Nyirenda says Malawians should not shy away from reporting misbehaving judges to authorities whenever there are questionable...

Close