Email a copy of 'Robbers hijack OPC vehicle, shoot one' to a friend * Required Field Your Name: * Your E-Mail: * Your Remark: Friend's Name: * Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries. Friend's E-Mail: * Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries. Image Verification: * Loading ... Sharing is caring! 0 shares Share Tweet Pin LinkedIn Email Print
what do you expect from this nkhalamba yoyanikidwa pa chingwe?????????????
Zimapheka akamayendetsa ena
Vytu lolamulilidwa ndi nkhalamba ndi choncho,munthu wa dementia angakuthandizeni??He has no idea.
Galimoto yaku OPC kupangangidwa Hijack kkkk ndie pali malamulo pamenepa kukanakhala kuti boma lathu liri ndimphamvu sibwezi muthu akutchinga galimoto ya atsogoleri athu kaya tiziona amalawi.
sata no more ndithu
Kodi mesa munkati DPP chitetezo? Boma lamayi citetezo kilibe mmm ai pano nde ndi worse
Basi tele eniake mukuti dzilibwino…Mapeto ake adzajacka officeyo ndi anthu omwe.musamakonde kuphethira….
DPP and Mlahklo team kuba !!!! Mutinyatsa nalo khalidwe lanuli.
Chilungamo!!Chitukuko!!Chitetezo!! Kaya china chija ndi chiyani?DPP woyeeeeeeee!!
Paja Boma ili chitetezo mchokhwima mpaka galimoto zikubedwabe? Ndiye Bola Mastenitu.