Email a copy of 'Satanist claimant arrested in Mzuzu: Malawi Police says he is trickster' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Satanist claimant arrested in Mzuzu: Malawi Police says he is trickster' to a friend
Business went as usual in the Capital City Lilongwe as Malawians held peaceful demonstrations to express anger over dwindling of...
EISHIIIH! “KUBA” SIMPLIFIED.
Mbava zapeza fomular.
chavuta pa malawi kuwerengana kwambiri mzanu asaiphule basi mwakhomerera asaaaa…. amene wafoilitsa movie uzafa imfa yowawa
Wina ndi uja amanamizira misala. Akaona galimoto ili ndi sticker ya TB Joshua amakaigwira ndikukhala ngati wachira. Fans ya TB Inkamupasa khusa heavy
A polisi nanu kusowa chochita2 pamenepa. M’tayeni pa 3 belo bax
Koma anthu enanu mukadali mtulodi yes,why comparing this thief with men of God? ambuye akukhululukire sukdziwa chimene ukunena,ukuwonetselatu kuti iwe ndiye mwana wake weniweni wa satana,serious and chimene ukukhalirabe ndi moyo pa dziko lino sindikuchidziwa komabe mulungu wathu ndi wachifundo amatisiyabe ndi moyo kuti tilape machimo athu onse,sintha m`bale wanga usanafe bcz zikuwonstselatu kuti nthawi yako ndiyochepa chonde lapa,this might be your last chance of repenting.
kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk mother fucn assholeeeeee!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!
Apa ndiye man munayiphulatu koma ndi ndani anakuwerenganiyo?kkkkkkE! pamalawi pakumvesa kuwawa!
Fanz ya ku kaya yayamba kuthaima eti? Kkkkkkk
Umphawi pa Malawi wafikapo. Eish…